iye amene a m idownload.branham.org/pdf/cha/cha63-1110e he that is in... · 2019-11-11 ·...

60
IYE AMENE ALI MWA INU Zikomo inu, M’bale Neville. Ambuye akudalitseni inu. Tiyeni tingokhalabe chiimire kwa mphindi chabe pamene tikupemphera. Tiyeni tiweramitse mitu yathu tsopano. Ndipo onse amene akufuna kuti akumbukiridwe mu pemphero ili, kwezani manja anu ndi kuti, “Ambuye, ndi ineyo.” 2 Mulungu Woyera koposaposa ndi Wachisomo, ife tikuwabweretsa anthu awa pamaso Panu, ndi zopempha zimene iwo ali nazo. Iwo apempha kuti akumbukiridwe. Ndipo, Ambuye, dzanja langa liri mmwamba nanenso. Ine ndikukupemphani Inu kuti mutichitire ife chifundo. Inu mukudziwa zosowa zathu, ndipo ife tikupemphera, monga Inu munatiphunzitsira ife kupemphera, “Ufumu Wanu udze. Kufuna Kwanu kuchitidwe pansi pano, monganso Kumwamba.” Atate, tikukupemphani usikuuno chifundo, ufulu wa Mzimu, kuti ife tikathe kubweretsa kwa anthu Uthenga wa Choonadi, ndi chimene ife tikukhulupirira kuti ndi Uthenga wa ora lino, kwa Mpingo Wanu. Ambuye, tikupemphera kuti ndife gawo la Mpingo umenewo umene uti udzaitanidwe utuluke mmasiku otsiriza! Atate, ngati ife sitiri gawo limenelo, ndiye mutiwululire ife chimene ife tingachite kuti tikhale gawo limenelo. Ndipo tipatseni ife chisomo, mphamvu, mu ora loyesa ili limene liri padziko lapansi kuti likayese iwo onse amene akukhala kuno. Tipatseni ife cha Mzimu Wanu Woyera, kuti utitsogolere ife ndi kutilondolera ife, kuti tikakhoze potsiriza, pamapeto, kubwera kwa Inu mu mtendere, chifukwa cha Moyo Wamuyaya uwo umene okhulupirira onse akhala akuwuyembekezera chiyambireni cha nthawi. Tithandizeni ife, Ambuye. Ife tikupempha mu Dzina la Yesu. Ameni. Inu mukhoza kukhala pansi. 3 Ine ndithudi ndiri wothokoza chifukwa cha mwayi wodzakhala kuno usikuuno—usikuuno, ndi chifukwa cha chisomo cha Mulungu chimene chaperekedwa kwa ife kudzera mwa Yesu. 4 Ndiyeno za—Uthenga mmawawu, tsopano, ine ndikufuna aliyense amvetsetse bwinobwino. Tsopano, ine ndikudalira kwa Mulungu kuti nthawi yake si imeneyo. Mukuona? Koma Uthenga ndi woona. Uthenga ndi woona. Iyo idzatero, iyo idzakhala nthawiina, ngati nthawi yake si imeneyo. Ndipo zikuwoneka mochuluka kwambiri kuti ndi nthawiyo, mpaka ine ndinamverera ngati Paulo wakale, amene anati, “Ine sindinaleke kukuuzani inu Uphungu wonse,” mwaona, chirichonse chimene chiti chidzachitike.

Upload: others

Post on 31-Jan-2020

0 views

Category:

Documents


0 download

TRANSCRIPT

Page 1: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU

Zikomo inu,M’baleNeville. Ambuye akudalitseni inu.

Tiyeni tingokhalabe chiimire kwa mphindi chabe pamenetikupemphera. Tiyeni tiweramitse mitu yathu tsopano. Ndipoonse amene akufuna kuti akumbukiridwe mu pemphero ili,kwezani manja anu ndi kuti, “Ambuye, ndi ineyo.”2 Mulungu Woyera koposaposa ndi Wachisomo, ifetikuwabweretsa anthu awa pamaso Panu, ndi zopemphazimene iwo ali nazo. Iwo apempha kuti akumbukiridwe.Ndipo, Ambuye, dzanja langa liri mmwamba nanenso. Inendikukupemphani Inu kuti mutichitire ife chifundo. Inumukudziwa zosowa zathu, ndipo ife tikupemphera, mongaInu munatiphunzitsira ife kupemphera, “Ufumu Wanu udze.Kufuna Kwanu kuchitidwe pansi pano, monganso Kumwamba.”Atate, tikukupemphani usikuuno chifundo, ufulu wa Mzimu,kuti ife tikathe kubweretsa kwa anthu Uthenga wa Choonadi,ndi chimene ife tikukhulupirira kuti ndi Uthenga wa oralino, kwa Mpingo Wanu. Ambuye, tikupemphera kuti ndifegawo la Mpingo umenewo umene uti udzaitanidwe utulukemmasiku otsiriza! Atate, ngati ife sitiri gawo limenelo, ndiyemutiwululire ife chimene ife tingachite kuti tikhale gawolimenelo. Ndipo tipatseni ife chisomo, mphamvu, mu oraloyesa ili limene liri padziko lapansi kuti likayese iwo onseamene akukhala kuno. Tipatseni ife cha Mzimu Wanu Woyera,kuti utitsogolere ife ndi kutilondolera ife, kuti tikakhozepotsiriza, pamapeto, kubwera kwa Inu mu mtendere, chifukwacha Moyo Wamuyaya uwo umene okhulupirira onse akhalaakuwuyembekezera chiyambireni cha nthawi. Tithandizeni ife,Ambuye. Ife tikupemphamuDzina la Yesu. Ameni.

Inu mukhoza kukhala pansi.3 Ine ndithudi ndiri wothokoza chifukwa cha mwayiwodzakhala kuno usikuuno—usikuuno, ndi chifukwa chachisomo cha Mulungu chimene chaperekedwa kwa ife kudzeramwa Yesu.4 Ndiyeno za—Uthenga mmawawu, tsopano, ine ndikufunaaliyense amvetsetse bwinobwino. Tsopano, ine ndikudalirakwa Mulungu kuti nthawi yake si imeneyo. Mukuona? KomaUthenga ndi woona. Uthenga ndi woona. Iyo idzatero, iyoidzakhala nthawiina, ngati nthawi yake si imeneyo. Ndipozikuwoneka mochuluka kwambiri kuti ndi nthawiyo, mpaka inendinamverera ngati Paulo wakale, amene anati, “Ine sindinalekekukuuzani inu Uphungu wonse,” mwaona, chirichonse chimenechiti chidzachitike.

Page 2: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

2 MAWU OLANKHULIDWA

5 Panali chinthu chimodzi chimene ine ndinachita mmawawu,chimene ine ndikupepesa kuti ine ndinanena izo. Ine—inendinatchula dzina la m’bale zimene ine ndikuganiza kuti ndizolakwika. Ine sindimayenera kuti nditero. Ine sindimatchulankomwe dzina la munthu; ndipo ngati tepiyo zingachitike kutiyafika mmanja ake. Ndipo ine ndikufuna kuti ndimuwoneiye ndipo ndiyankhule naye, chifukwa ine ndikuganizam’baleyo, mwamuna wopambana, mwamuna wabwino amenewalalikirapo pano pa guwa ili, M’bale David duPlessis.Ndipo ine sindimatanthauza kuti nditchule dzina lake. Inendimadandaula ndi Uthenga, ndi zina zotero, zakuti nangabwanji ngati nthawiyo itakhala pano, ndipo ine ndinatchuladzina la m’baleyo. Ine sindimachita zimenezo. Ine ndikupepesakuti ine ndinachita zimenezo. Ine ndimamukonda M’bale DavidduPlessis. Iyeyo ndi m’bale wathu, ndipo ine—ine ndikuganizakuti munthu wophunzira ngati ameneyo amayenera kukhalawophunzitsidwa bwinoko mu Lemba.

Ine ndikuuzani inu chimene icho chiri. Ndi, zokambiranazimene David ndi ine tinali nazo…6 Iye nthawiina anayankhula m’malo mwanga mumisonkhano. Iye analalikirapo kuchokera pa guwa lomwelino, kapena tchalitchi chakale, pompano pa guwali. Ndipom’bale wake, Justus, anali wotanthauzira wanga ku SouthAfrica, kumene ine ndikubwererako. Ndipo iwo amachokeraku banja labwino, khomo la Chipentekosite, munthu wabwinokwenikweni. David anali, ine ndikukhulupirira, wapampando,nthawi ina, waWorld Pentecostal Assemblies, ndi ku PentecostalWorld Conference. Iye anali m’modzi wa apampando.Ndipo kenako iye anadzabwera ku United States ndipoanadzakhazikika, ku Texas, ndi M’bale Gordon Lindsay, ndipoatatero anangoyamba kulalikirammalo osiyanasiyana.7 Koma chimene icho chinali, pamene ine ndikuganizakuti m’bale wathu wofunika analakwitsira; chimodzimodzimonga mmene inenso ndikhoza, kapena wina aliyenseyo; iyeanayamba kuchita ndi apamwamba—ndi—apamwamba. Iyeanakhala akukamba za Princeton University ndi malo ameneamamuitana iye, kumaganiza kuti iye amachita chimene chinalicholondola, ndipo iye amayika utuchi mmakinawo; mwaona, ndikumasangalala nazo chomwecho!

Ngati kuti sizokhazo, koma a Full Gospel Business Men,amene amathandizira msonkhano wanga, padzikolonse—konsekonse. Mukuona? Ine—ine ndimawakonda amunaamenewo, mwaona, koma ine ndithudi sindigwirizana nawoiwo pa mfundo zimene iwo—iwo ali—iwo ali…Iwo a—iwo achoka kumene, mfundo zawo, zimene iwo anayambanazo, ndipo tsopano iwo akungokhala ngati bungwe linalirilonse kapena chirichonse. Mukuona? Ndipo chimene izoziri, iwo sakuyesetsa kuti angokhala achipentekosite, koma iwo

Page 3: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 3

akuyesetsa kumasakaniza chipentekosite ndi zina zonse za izopamodzi.8 Ndipo zikuwoneka kwa ine ngati kuti M’bale duPlessis,munthu wopambana, wabwino monga choncho, amayenerakudziwa mokwanira za Lemba kuti pamene iye akumuwonanamwali wopusa akuyesera kuti adzagule Mafuta, nthawi yatha.Mukuona? Kumbukirani, pamene iye anabwera kuti adzaguleMafuta, kunalibeko Mafuta amene anatsalira. Amenewo ndiyeMalemba. Ndipo iye anati, “Tigaireniko ife Mafuta anu,” kwaMpingo, koma iye sanapatsidwe Iwo. Iye akhoza kulumpha-lumpha, kuyankhula mmalirime, ndi zinazonsezo, koma, mongamwa Mawu a Mulungu Mwini, iye sanapatsidwe Iwo. Ndipoiye anali kunja uko mu mdima wakunja; ndipo uko kunalikulira, kusisima, ndi kukukuta kwa mano, pamene Mkwatibwiwosankhidwa anali atapita kale. Na—namwali wochenjera analindi Mafuta mu nyali yake.9 Tsopano, ine—ine ndikudziwa munthu wina, chinachakechimene chinachitika basi tsiku lina. Chimene chiri, ndi chakutianthu abwino awa, mwaona, akupita pang’ono, inu mukudziwachimene ine ndikutanthauza, kugwira pang’ono pa anthu. Ndipochinthu choyambirira inu mukudziwa, iwo amamverera kutindi Mulungu ameneyo amene akuchita zimenezo. Ndipo nthawizambiri, ameneyo amakhala mdierekezi akuchita zimenezo.Mukuona?10 Yesu anali nawo mwayi wobwera pamaso pa Herodi; Iyeanali nawo mwayi wobwera pamaso pa ambiri, ndipo iwoankafuna kuti amugwiritse ntchito Iye ngati chiwonetsero.Mukuona?

Ndizo zonse zimene iwo akuyesera kuti achite kwaApentekosite. Apentekosite anatuluka mu zinthu zimenezo, kutiadzakhale osiyana. “Ndipo monga nkhumba ku matope ake, ndigalu ku masanzi ake, akutembenuka kubwereranso komwe kujakachiwiri,” ndipo tsopanomuBungwe la Ecumenical. Mukuona?Ndi zoipa kwambiri. Ndi za manyazi.11 Mulungu ndisungeni ine ndikhale wamng’ono ndiwodzichepetsa, kuchitira kuti Iye athe kuulula Choonadi Chake.Mukuona? Ine sindimafuna kuchita zimenezo; sindimafunamagetsi onyezimira, ndipo sindimafuna zonyezimira ndizothwanima kwa dziko. Ndiloleni ine nditenge njira ndi ochepaonyozeka a Ambuye. Ndiloleni ine ndikhale ndiMawu.12 Tsopano kukamba za Ecumenical Council kugwirizana ndiVatican. Kodi inu mukukhulupirira kuti iwo angagwirizanepa Mawu? Iwo atha kutero pa bungwe, koma iwo sangateropa Mawu. Mukuona? Uko nkulondola. Kotero palibechirichonse choti tizilekerera. Mukuona? Bungwe, zonsezo ndichimodzimodzi, chirichonse chikufanana; izo ziri mu mzeremwangwiro, mayi ndi mwana wake. Koma pamene zifika ku

Page 4: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

4 MAWU OLANKHULIDWA

Mawu awa, ine ndimakhala wotsutsa zolimba Chimethodistndi Chibaptist ndi Chipresibateria, chimodzimodzi mongandimatsutsira Chikatolika, chifukwa ndi mayi ndi mwanawamkazi, monga mwa Mawu awa. Ndi Mawu awa amene inendimaima nawo,mwaona,Awa, Mawu aliwonse a Awa.13 Tsopano, m’bale wofunika uyu, iye ndi mkazi wake ndiabwenzi anga apafupi. Ambiri a inu munawona magazini,mmene zinakhalira kuti m’bale wofunika uyo, wotumidwandi Mulungu anamulola bwanji mkazi wake…Winawakeanamuuza iye kuti akuwoneka ngati Jacqueline Kennedy, ndipomwathengo iye anameta kametedwe kopambana kotchuka ndichinthu. Ndi chiyani chimenecho? Iye akuyanjana ndi anthu amtundu umenewo, nthawi zonse, ndipo potsiriza…

Mwamuna wabwino akatenga mkazi woyipa, iye mwinaamasanduka mkazi wabwino kapena…ine ndikutanthauza,mwamuna wabwino akatenga mkazi woyipa, iye mwinaamasandukamkazi wabwino kapena iye amasandukamwamunawoyipa. Mundisonyeze ine azimzanu, ine ndikuuzani inu yemweinu muli. Mukuona? Mbalame za nthenga zofanana, zimaulukiralimodzi. Mukhale kutali ndi zinthu zonyezimira!14 Ine ndinakwera mu mgodi, tsiku linali, pamwamba pomwepa mapiri a Arizona ndi—ndi mzere wa Mexico. M’baleSothmann ndi ine, wakhala apayu, tinali pamwamba apolimodzi. Ndipo ine ndinafika pamenepo ndipo ndinakumbamulu wa chimene…Iye amawoneka ndendende ngati golide.Koma njira yokhayo imene iwe ungadziwire kuti iye si golide, iyeamanyezimira bwinoko kuposa golide. Iye amanyezimira. Ndipogolide samanyezimira, iye amawala. Mukuona? Ndipo ameneyoamatchedwa, “golide wopusisa.” Mtengo wake sumakwanamochuluka ngati mwala umene umakhala mmenemo. Iwoumatchedwa chitsulo cha galasi. Ine ndikuganiza, mu a—a…Asayansi amanena kuti madzi ndi maasidi owukha, ndizinthu, sizimafika pamenepo mokwanira kuti zikamulimbitseiye ndi kumubweretsa pamalo akuti apangike kukhala golide.Chotero iye—iye amanyezimira bwinoko, koma iye samakhalandi zipangizozo mmenemo.

Ndipo basi ndi momwe ziliri ndi Chikhristu chodzipangitsachochuluka, mwaona, icho chimanyezimira, ndipo ngatiHollywood. KomaMpingo umawala ndi Uthenga.15 Tsopano, mlongo wina pano, Billy amandiwonetsa kumeneine, anachita zabwino kwambiri kuti anapita ndipo anakatengaLife magazine iyi, chithunzi ichi, ndipo anakachikulitsa icho,cha Angelo asanu ndi awiri chija, ndipo anachijambula ichondi kuchitumiza kwa ine. Chithunzi chake ndi chimenecho.Ndipo tsopano ngati inu mungazindikire apa, pamene iwoamanyamuka, akukwera pobwerera, pamene Angelowo analiatabweretsa Uthenga Wawo, izo zinali mmaonekedwe a

Page 5: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 5

piramidi; ndendende basi zimene ine ndinakuuzani inu,miyezi itatu izo zisanachitike, mmene izo zikanadzachitikira.Nkulondola uko? [Osonkhana akuti, “Ameni.”—Mkonzi.]

Ndipo Mngelo wozindikirika, wokhala ndi mapiko Akemmbuyo kumbali, mmbuyo, akugonera chammbuyo, inumukukumbukira? Ndipo ndinati, “Iye anali ndi mutu Wake…akubwera paliwiro ili.” Kodi inu simukuwawona ngakhalemapikowo pamenepo? Ndipo ndi uyo Mngeloyo pamenepo,ndendende basi mmene izo zinanenedwera.16 Tsopano, Mulungu yekha ndi yemwe angachite zimenezo.Iwo ali nacho chithunzicho kuno, aponso, cha mkazi ameneanati…Nthawi zambiri, anthu amati…17 Mu ku—ku kuzindikira za mumtima, ndimati, “Munthu uyuwaphimbidwa ku imfa, mthunzi wakuda.”18 Tsopano iwo amati, “Chabwino, iye akungonena zimenezo.”Mwaona, amenewo ndi anthu amene sangapite njira yonse,iwo samawona zimenezo. Iwo akhoza kufuula ndi iwe, iwoakhoza—iwo akhoza kuyankhula ndi iwe; koma pamene zifikapokhulupirira kwenikweni zonse, solo yonse ndi thupi, iwoamalephera kuchita zimenezo.

Chotero, koma inu mukuona, ngati Mulungu ali muzimenezo, ndipo ndikunena Choonadi, ino ndi nthawi yotsirizaya mbiriyakale. Ano ndi mathelo a mbiriyakale ya dziko.Kuno ndi kutsekera. Sipadzakhalanso nthawi, tsikulina.Mulungu akutsimikizira chirichonse, zonse ziwiri mwauzimundi mwasayansi.19 Pamene ine ndinati, mnyamata wamng’ono, “Lawi laKuwala, linawoneka ngati nyenyezi.”20 Ndi angati akukumbukira, nthawi zakale, iwo ankakondakulitchula Ilo “Nyenyezi?” Pamene Ilo linadzawonekera kumusikuno pa mtsinje, pamene Iye anati, “Monga Yohane M’batizi,anatumidwa…”21 Tsopano, potsiriza, Ilo linatsika, ndipo chithunzichinajambulidwa cha Ilo. Ife tinkakhala nacho chimodzi muno,penapake. Eya, iwo akuti icho chiri apo pa kona; Ine sindikuthakuchiwona icho. Zinatsimikiziridwa mwasayansi kuti ndiChoonadi.22 Ndipo tsopano, ndipo kunena kuti anthuwo“anaphimbidwa.” Tsopano, apa panali mkazi, chithunzi.Ndi icho apo, chabwinobwino, monga ngati chithunzi chinachirichonse;mongawina kujambula ichi, makina. Ine ndinati…Munthuyo amadabwa za icho. Ndipo ndinati kwa mkaziyo, “Inumwaphimbidwa ku imfa, ndi khansa. Pali mthunzi wakuda.”Iye anapotoloka ndipo anajambula chithunzicho. Mkaziyowakhalapo kuno kudzachitira umboni, ndipo mwinamwakeadakalibe kuno usikuuno,mmene ine ndikudziwira.Mukuona?

Page 6: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

6 MAWU OLANKHULIDWA

Tsopano, apo pali mkazi ali ndi chonga ngati chophimbachakuda pa iye. Chabwino, tsopano, ndi kumenekokutsimikizira kwa sayansi kuti ndi choonadi. Ndipo pomwepomkaziyo atalengezedwa kuti “alibwino,” iwo anajambulachithunzi, ndipo iwo panalibepo apo. Nchiyani chinakhudzagalasilo ndiye? Ndipo nchiyani chinachokapo, icho sichinatero—panalibepo pa galasipo pamene zimalengezedwa kuti iyewachiritsidwa? Mukuona?

Tsopano, nditaima pano, ndinakuuzani inu kuti Angeloakubwera.23 M’bale Fred, pokhala mmodzi…Ine ndinamuwona M’baleFred kanthawi kapitako. Ine ndimaganiza kuti iye analipompano, koma ine ndamuphonya iye penapake. Oh, kumbuyokuno, uko nkulondola. Iye anali ataima mkati mwa—mailosiawiri, kapena mailosi ndi theka, kapena mamailosi awiri,ndi pamene ine ndinali; anamva kuphulikako, ndikumvereramwalawo, ndi china chirichonsecho, pamene izo zimapita.Nkulondola uko, M’bale Fred?

Ndipo apo panali Angelo amene anatumizidwansondi Uthenga umenewo. Ndipo pano izo ziri ngakhale mumaonekedwe a piramidi, monga ine ndinakuwonetserani inuchimene izo ziti zidzakhale kuno, ndinakuuzani mmene Iwo atiazidzaimira, ine ndisananyamuke.

Chithunzi pambuyo pa chithunzi, kudutsa dzikoli,anajambula izo, kudutsa mpaka ku Mexico, kukhala mamailosisate kupita mmwamba ndi mamailosi twente seveni chopingasa.Ndipo kupita mmwamba kwambiri mwakuti ngakhalechinyontho kapena kalikonse…Chinyontho sichiyendakupitirira pafupifupi mamailosi eyiti kapena naini, kupitammwamba, ndiye iwo anapita ku malo kumene kulibekochirichonse chimene chingapange chinyontho. Mukuona? Ndipoichi chinali, ine ndikuganiza ichi chinali mwina mamailositwente seveni kupita mmwamba ndi mamailosi sate chopingasa,kapena mwina icho chinali—icho chinali twente-…kapenamamailosi sate kupita mmwamba ndi mamailosi twente-seveni chopingasa, chimodzi mwa izi. Life magazine inalembazimenezo, kapena Look. Inali iti, Look kapena Life? Life, Lifemagazine. Ine ndikuganiza, ya, Meyi 17. Ndi choncho.24 Tsopano ndi zimenezo apo, mwasayansi, chitsimikizochakuti ichi ndi Choonadi, chotero chomwecho ife—ifesitidandaula ndi kuti kaya ndi Choonadi; ziwiri zonsemwasayansi, ndi mwauzimu, chimene chinanenedwachinadzachitika. Chotero, Uthenga wa Zisindikizo ZisanuNdi Ziwiri, mu kutsekera kwake, ndiwo Uthenga wa Baibulolonse. Zisindikizo Zisanu Ndi Ziwiri zikutsekera ChipanganoChatsopano ndipo chasindikiza icho. Izo ndi zoona. Tsopano, ifetikudziwa kuti izo ziri, mwa maneno a uneneri, mwa sayansi,

Page 7: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 7

ndi mwa Mawu. Zitatu zaperekera umboni kwa izo, kuti izo ndiChoonadi.25 Chotero, ife tikudziwa kuti ife tiri panthawi yotsiriza. Ife tiripano. Ine sindikudziwa kuti ndi patali bwanji, ine—ine…Iyesadzatilola kuti ife tidziwe zimenezo, chifukwa Kudza Kwakekudzakhala “ngati mbala usiku.” Amzanga, m’bale wanga,mlongo, tiyeni tingokhala okonzeka, mulimonsemo. Tiyenitingodzisunga tokha. Mukuona? Chifukwa, dziko lidzakhalalikupitirirabe. Iwo sadzadziwa nkomwe kuti chachitika ndichiyani. Pamene zitseko za chifundo zatsekedwa, alalikiadzakhala akulalikirabe chipulumutso, adzakhala—adzakhalaakuwapangitsa anthu kuti alape, kumapitirirabe chimodzimodzibasi monga izo zimachitikira nthawizonse. Izo zinatero mumibadwo inayo, ndipo izo zinatero mu…Izo zitero mum’badwo uno.

Ndipo Mkwatulo udzakhala wodzidzimutsa kwambiri ndiwamsanga kwambiri, mwakuti dziko silidzawasowa nkomweiwo, kuti iwo apita. Kulondola. Iwo sadzadziwa kalikonse za izo.Iye akubwera ndi kudzamuzembetsera Iye kutali. Iwo udzakhalautapita, iwo sadzadziwa kalikonse za izo.

Chotero, mukhale mu pemphero. Muzindipempherera ine.Ine ndizikupemphererani inu. Ife sitikudziwa ndi liti oralimenelo liti lidzakhale, koma ife tikukhulupirira izo zichitikaposachedwapa.Mukhale kutali ndi zinthu zonyezimira.Mukhalendi Uthenga, mwaona, mukhale pomwepo tsopano, ndipozipempherani.26 Tsopano, Billy wandilembera ine kalata pano, kapenaka cholembedwa kani, ndipo akuti winawake akufuna kutiadalitsitse mwana. Ngati ziri chomwecho, (ndi choncho?)kwezani mmwamba dzanja lanu, ngati ena…Eya, makandaawiri. Chabwino, abweretseni iwo pompano. Ndipo M’baleNeville…Ndipo ine ndikudabwa ngati mlongo wathu palimba angabwere apa kwa mphindi chabe, pa kudalitsitsa kwamwanayo. Ife sitikufuna kuti tisiye chirichonse.27 Tsopano, kumbukirani, nthawi ino mawa usiku, Ambuyeakalola, ine ndidzakhala ndiri ku Mzinda wa New York. Ndipoife tikupita kumeneko ku bwalo la nkhondo, kuti “tikamenyenkhondo yabwino ya Chikhulupiriro.”28 Chotero pomwe pano, mlongo, ngati inu mungatero.Kutsogolo komwe kuno, ndipo ine ndiwanyamula iwo. Inde,amayi. Zikomo inu. Ndipo tsopano ife tiri…29 Ndi angati azindipempherera ine? [Osonkhana akuti,“Ameni.”—Mkonzi.] Tsopano, Mulungu akalola; chimene, inendikuyembekeza Iye watero; Lamlungu, pakatha sabata…Ngati ziribwino ndi M’bale Neville. [M’bale Neville akuti, “Ziribwino.”] Lamlungu, pakatha sabata, ine ndidzabwereranso

Page 8: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

8 MAWU OLANKHULIDWA

kachiwiri, pa ulendo wanga waku Louisiana, ndipo ndidzaimakuti ndidzakhale ndimsonkhano kuno ku tchalitchi. [“Ameni.”]30 Ine ndikufuna ndikuthokozeni inu nonse chifukwa chachifundo chanu. Dona uja amene ananditumizira ine suwitiuja uko, ine—ine ndikuyamikira zimenezo. Sindikudziwa kutidonayo anali ndani. Winawake ananditumizira ine bokosi lasuwiti ndi kamba wina monga choncho. Izo ndithudi zinali,zokoma kwenikweni. Izo zandikhutitsa ine pakali pano,ndipo ine—ine ndikukuthokozani inu. Ndipo inu mukuganizakuti zinthu zazing’ono zimenezo sizitanthauza mochuluka?Izo ndithudi zimatero; kosonyezera kakang’ono. Ndipoosiyanasiyana akupereka timphatso tawo tating’ono ta chikondi.Ndipo akumamuwonetsa Billy Paul, ndi kumapereka izo, ndizinthu. Ine—ine ndikulandira izo, mwaona. Inu simukudziwamomwe ine ndimayamikirira izo! Mulungu akudalitseni inu.Ine ndikakumbukira izo, mwaona, ndi mochuluka bwanjimomwe Iye amakumbukirira izo. “Mochuluka momwe inumwachitira kwa aang’ono Anga awa, inu mwachitira izo kwaIne.” Mukuona? Tsopano, chifundo chimawonetsedwa pamenechifundo chaperekedwa.31 Tsopano, ife tiri ndi ana ena abwino pano. Kodi inu…Ine ndikufuna kuti inu mukhale pamenepo ndipo muziyimbaBwezatu, kenako. Chabwino, abale inu mubwere kuno minitichabe.

Mai, apa pali woyamba, timaso ta bulauni tikuyang’anapa ine, ndi kumwetulira kwakukulu, kokongola. Mtsikanawamng’ono, ndi ndani…[Amake akuti, “Sharon Rose. SharonRose.”—Mkonzi.] Sharon Rose, limenelo ndi dzina lopambanakwa ine. [“Ife tinamutcha iye, M’bale Branham, potengerawanu.”] Munatengera mtsikana wanga wamng’ono ameneanapita. [“Ife tinamutcha iye asanabadwe nkomwe, M’baleBranham.”] Munamutcha iye asanabadwe. Ngati iye adzakhalemtsikana wamng’ono, inu mukanati mudzamutche iye SharonRose. [“Ife tinali otsimikiza kuti iye adzakhala mtsikana. Iyeamayenera kuti akhale.”] Amayenera kuti akhale. [“Sharon RoseGoodman.”]

Inu mukudziwa chiyani? Ine sindikudziwa kuti inumukudziwa chimenecho kapena ayi; ngati mkazi wangaakanakhala kuti ali pano, iye mwinamwake akanatsala pafupikuti akomoke. Uwu ndi mtundu womwewo wa diresi limenemtsikana wanga wamng’ono anavala pa kumudalitsitsa, SharonRose wamng’ono. Uyu mwina akhoza kukhala…Uyu atakhalamoyo; pamene,Mulungu anamutengerawangammwamba.

Kodi dzina lanu la kumapeto ndi chiyani? [Amakeakuti, “Goodman.”] Mayi ndi…Kodi mukuchokera kuno mumzindawu? [“Chicago.”] Chicago. M’bale ndi Mlongo Goodman,Mulungu akudalitseni inu.

Page 9: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 9

Inu mukudziwa, Sharon Rose wanga wamng’onoankawoneka ngati ameneyo. Ine sindikuganiza kuti pali aliyensepano amene akukumbukira mmene iye ankawonekera. Iye analindi maso aang’ono a bulauni ngati awo, ngati amayi ake,mtsikana wamng’ono wokoma kwenikweni wa tsitsi lakuda.Basi pafupifupi…

Kodi mwanayu ndi wamkulu bwanji? [Amake akuti, “Miyezifaifi.”—Mkonzi.] Miyezi faifi. Iye anali ndi miyezi eyiti pameneMulungu anamuitanira iye kumwamba. Ine ndinamuwona iye,pang’ono zitachitika zimenezo. Inu mukuidziwa nkhaniyo. [“Ifetiri nayo iyo kwathu, pa tepi.”] Inumuli nayo iyo kwanu, pa tepi.

Sharon Rose amachokera ku Mawu. Ine ndinalitembenuzailo, kuchokera ku, “Duwa la Sharon.” Ndipo Iye amafunamwana, wonga iwo, pa guwa Lake, chotero Iye anamutengaiye. Mukuona? Ndipo ine ndidzakakhalanso naye iye. Sharonwanu wamng’ono akhale moyo kuti akwaniritse moyo umene iyeakanati akhale kuno pa dziko lapansi. Ndipo iye adzakakhalendi inu ku Ulemelero, monga mmene ine ndikumverera kutiSharon wanga adzakakhala ndi ine.

Inu muli bwanji? Mukuona? Inu mukakamba za kanthukakang’ono kosangalatsa, tamuonani uyu! Iye akungomwetulirayense.

Tiyeni tiweramitse mitu yathu.Wokondedwa Mulungu, pamene ine ndagwirizira chuma

chaching’ono ichi, Sharon Rose wamng’ono. Inu mukudziwamu mtima mwanga, Ambuye, chimene ine ndikuganiza, choteroine sindikusowa kuti ndifotokoze izo. Wodala akhale AmbuyeMulungu Amene amapereka ngale zazing’ono izi ku mitimayathu! Mudalitse khomo la a Goodman ili. Mulole makolowaalemekezedwe, chimene iwo ali, pokhala ndi ngale yotereyi pakhomo. Mulole iyo ikakhale pakhomo pawo, Ambuye. Ndipongati kulimawa,mudzampange iyemkaziwaulemuwamawa.

Ndipo tsopano, Ambuye Mulungu, pomvera chimeneInu munatituma ife, mwa chitsanzo Chanu, kuti tizichita,Inu munatengera tiana tating’ono mmikono Mwanu ndipomunatidalitsa ito, ndipo munati, “Mulole ana aang’onowaabwere kwa Ine.” Ndipo iwo abweretsa mwanayu kwa ine,pokhala wantchito Wanu, monga Inu munanenera kuti atumikiAnu azipitiriza ntchito Yanu. Ndipo pano paima antchito Anu,M’bale Neville, ndi M’bale Capps, ndi ineyo. Ndipo tsopano,Ambuye Mulungu, kuchokera mmikono ya abambo ndi amayi,ife tikumpereka kwa Inu Sharon Rose Goodman wamng’ono,amene ife tikumudalitsira ku moyo wa utumiki, mu Dzina laYesu Khristu. Ameni.

Mulungu akudalitseni inu! [MlongoGoodman akuti, “M’baleBranham, ife tirinso ndi faifi ena ku nyumba, atsikana awirindi anyamata awiri.”—Mkonzi.] Asanu ang’ono, pambali pa uyu!

Page 10: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

10 MAWU OLANKHULIDWA

[“Inde.”] Nzokoma bwanji! Mulungu akudalitseni inu, M’baleGoodman. Mulungu akudalitseni inu, Mlongo Goodman. NdipoAmbuye amudalitse Sharon wamng’ono!

Inu muli bwanji, m’bale? Tsopano tiyeni tiwone, ine—ine…Arnett. [Bambo akuti, “Arnett.”—Mkonzi.] Arnett.Arnett, nkulondola uko. [“Tinamutcha potsanzira—tinamutchapotsanzira inu.”] Kodi ndi choncho? William, William Arnett?[“James William Arnett.”] James William Arnett. Uyu ndimnyamatawabwino. Inumukudziwa, zinthu zina ife tikufanana,iye ndi ine, mainawo; kale, ndipo kenako tsitsi lathu likugonamofanana, inu mukuona. Iye ndi mnyamata wabwino, Jimmy.Ndikuganiza ndi chimene inu mumamutcha iye, James?[“James.”] James, ndiye, chabwino.

Ndikudabwa ngati ine ndingamunyamule iye? [“Iye akhozakukupulumuka iwe.”] Ine sindikudziwa. Tsopano, Jimmy,chabwino, ife ndi abwenzi enieni. Inu mukudziwa zimenezo,sichoncho inu? Chabwino.

Tiyeni tiweramitse mitu yathu.

Ambuye Mulungu, Inu mwalidalitsa khomo ili, khomola Arnett ndi mnyamata wamng’ono wabwino uyu. Ndipoine ndikupemphera kuti Inu mudalitse bambo ake, amayiake, okondedwa ake. Iwo ndi Akhristu. Momwe kuti bamboake anamenyera molimba kwambiri, ndudu zija ndi zinthuzosiyanasiyana, kuyambira…Tsiku lina izo zinadzadzera,“PAKUTI ATERO AMBUYE.” Iye anali ngati mkazi ameneanali wokakamira kuti akafike kumeneko. Ngakhale geniyake imamukanika iye, ndipo chirichonse chinkawonekakuti chikukanika, iye anatengabe gawo la ndalama zakendipo amadikirira kuyankhulana kwapadera pambuyopa kuyankhulana kwapadera, kufikira mmawa wina izozinadzachitika. Iye ankakhulupirira kuti izo zidzatero.

Tsopano iye akumubweretsa mnyamata wamng’ono uyuamene Inu mwamudalitsa naye iye, O Mulungu, chipatso chachilumikizano chawo. Ine ndikumudalitsa JamesWilliam Arnettwamng’ono uyu, mu Dzina la Yesu Khristu. Mpatseni iye moyowautali. Mumpange iye mwamuna woyenera wa Uthenga Wanuwa mawa, ngati kuli mawa. Ndipo, potsiriza, mu Ufumu umeneuli nkudza, mulole ife tidzakakhale uko limodzi. Ine…atumikiAnu, ife tikuikamanja athu pa iye ndipo tikumudalitsira iye kwaYesu Khristu, kumoyo uwuwa utumiki. Ameni.

Akudalitseni inu. Mulungu akudalitseni inu, m’bale. Tatsalandi awiri ena? Awa ndi omwe aja. Chabwino.

Ine ndikukhulupirira iwe ukhoza pafupifupi kundinyamulaine, mmalo mwakuti ine ndikunyamule iwe. Uyu ndi…[M’baleArnett akuti, “Uyo ndi—uyo ndi Al.”—Mkonzi.] Alfred, ndi Alndi Martha. Mungolola osonkhana, ine ndimakonda kuti iwo

Page 11: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 11

aziwona ana. Ine ndikuganiza, pamene iwo akadali aang’ono,achichepere, iwo amakhala okoma.

Tsopano tiyeni tiyike manja athu pa iwo.Momwemonso, Mulungu Wamphamvuzonse, ife antchito

Anu, tikuika manja athu pa ana awa, m’bale wamng’ono ndimlongo wa mnyamata wamng’ono uyu amene tangomudalitsitsakumene pano. Ife tikuika manja athu pa iwo ku—kuwadalitsa,kuchokera kwa mayi ndi bambo, kupita mmikono ya YesuKhristu, kumoyowautumiki,muDzina la YesuKhristu. Ameni.

Mulungu akudalitseni inu, Al ndi Martha. Mlongo, zabwinokwenikweni kukuwonaninso inu. Ambuye akhale nanu.

Mzanga wamng’ono uyu, mai, iye ndi mnyamata wabwino.Ine ndinkakonda kumatha kuligawa tsitsi langamonga choncho.Mukuona? Dzina lake ndi ndani? [Bambo akuti, “Terrell KeithWalker.”—Mkonzi.] Ke-…[“Terrell Keith Walker.”] HerrellKeithWalker. Mnyamata wabwino bwanji!

Ine ndikudabwa, ine sindikudziwa basi, mwaona. Iyeakuyang’ana pa ine ngati kuti iye angathe. Ndikudabwa ngatiine ndingamunyamule iye? [Khandalo likuyankhula—Mkonzi.]Nkulondola uko, Keith? Oh, iye ndi mnyamata wabwino.Ndithudi. Kodi ameneyo si mnyamata wamng’ono wokondedwa?Herrell. [Amake akuti, “Terrell.”] Herrell, Terrell KeithWalker.

Mulungu Wamphamvuzonse, kuchokera mmikono yamakolo kupita mmikono ya Yesu Khristu, Terrell Keith Walkerwamng’ono, ife tikuyika manja athu pa iye mu kumudalitsitsirakwa Mulungu Wamphamvuzonse. Monga momwe bambo ndimayi akufunira kuti khanda ili likaleledwe mu malangizoa Mulungu. Ngati kuli mawa, mudzampange iye adzakhalewantchito woyenera kudalitsidwa uku, pakuti ife antchito Anutikuika manja athu pa khanda ili ndipo tikumudalitsitsira iyekwa Ambuye Yesu Khristu. Ameni.

Akudalitseni inu, M’bale Walker. Kodi awa ndi MlongoWalker? [Mlongo Walker akuti, “Inde, bwana.”—Mkonzi.] Ndizabwino kwenikweni. Inu muli ndi mnyamata wabwino, ndipoMulungu akudalitseni inu.

[M’bale Gramby akuyankhula ndi M’baleBranham—Mkonzi.] Chabwino, bwana. [M’bale Grambyakupitiriza kuyankhula.] Eya. [“Ndipo munampemphereraiye pamene iye anabadwa. Iye anabadwa ndi mfundo musagwada zake. Ndipo inu munampempherera iye, ndipo ichochinachoka pomwepo.”] Mtsikana wamng’ono uyu, ndi M’baleGrimsley wathu…[M’bale akuti, “Gramby.”] Gramby. Ine—ine ndimawasokoneza amenewo. Ine ndiri ndi M’bale Grimsley,ine ndimakhala ndikuganizira…M’bale Gramby akubweretsamtsikana wamng’ono uyu. Ndipo pamene iye anabadwa,iye anali ndi mfundo yaikulu pa nkhope pake. Ndipo inendinamupempherera iye, ndipo mfundoyo inasunthapo. Ndipo

Page 12: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

12 MAWU OLANKHULIDWA

tsopano iwo akufuna kupemphera, chifukwa…Kodi makolowondi Akhristu? [“Si Akhristu.”] Iwo si Akhristu. Ndipo iwoakuwopa kuti mzimu woyipa ukumutenga mwanayu, ndipoiwo akufuna iwo uchotsedwepo.

Tiyeni tipemphere.Ambuye Yesu, pa mwana wamng’ono uyu, pamene iye

watsamira pa guwa…Chimene, Inu mwawonetsa chisomo,kumuchotsera mfundo ya chophuka mkamwa mwake. Tsopanomzimu woipa ukuyesera kuti utenge moyo wa mwanayu.Nzosakayikitsa koma kuti Inu mukhoza kudzamugwiritsantchito mtsikana uyu, ndipo mukukonzekera kuchita zimenezo,ndipo Satana akuyesetsa kuti afooketse dongosololo. Chotero,ife tikumulamulira Satana, mu Dzina la Yesu Khristu, kutiachotse ake—manja ake ndi iyemwini kutali ndi mwana uyu;pamene ife tikumupereka iye kwa Ambuye Yesu Khristu, kwaulemelero wa Mulungu. Ameni.

M’bale Gramby, inu mukhulupirire. Mwanayu ndiwamng’ono kwambiri kuti akhale ndi chikhulupiriro, komazitheka.32 Ine ndimamkonda Iye. Si choncho inu? [Osonkhana akuti,“Ameni.”—Mkonzi.] Iye ndi wodabwitsa.

Tsopano, aliyense, ine ndinalonjeza usikuuno kuti inendikhala nditatuluka pofika hafu-eyiti, chotero izo zikundipatsaine theka la ora. Ine sindikudziwa tsopano za izo. Ine ndikhozakuchedwerapo pang’ono kuposera pamenepo. Koma tiyeni ifetsopano…33 Ndine wokondwa kumuwona M’bale Dauch pano mmawauno. Ndipo ine sindikudziwa kumene munthu winayo wapita;koma mmawa uno, ngati iye anakhalapo ndi wofanananaye, panali munthu amene anakhala kumbuyo komwe uko,anali wofanana mwangwiro ndi iye. Ine ndinati, “M’baleDauch ndi uti?” Ine ndinayang’ana mmbuyo ndi mtsogolo,ndipo ine ndinali pafupi kuchinena icho; ndipo ine ndinalinditakulungidwa kwambiri mu Uthenga. Inu mukudziwa,M’bale Dauch, inu mukuwoneka chimodzimodzi monga mmeneinu mumawonekera nthawizonse. Ndine wokondwa kwambirikumuwona iye mmene akuwonekeramu.34 Posachedwapa, ine ndinali ndi kuimbiridwa kuchokerakutali ku Tucson, kuti ndimupempherere iye, kutichinachakenso chinali chitachitika kwa iye. M’bale Dauch ali,ine ndikuganiza, nainte kapena nainte-wani. Ndi wausinkhuwa zaka nainte, ine ndikukhulupirira, kapena nainte-wani.Ndipo thupi lako limafooka. Koma, “Zochuluka ndi zosautsaza olungama, koma Mulungu amamuwombola iye kuchokamu zonse izo.” Ndipo nthawizina, pamene thupi lifika pamaloakuti ilo silingathenso kuzigwira pamodzi, ine ndikudziwaIye akugwirizira ku Dzanja. Ngakhale chigulumwa cha dothi,

Page 13: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 13

Mulungu analonjeza kuti adzachidzutsanso icho, mu masikuotsiriza. Ndipo ndine wothokoza kwambiri.35 Ine ndikukumbukira M’bale Dauch, pamene iye anabweramu dziwe kuno kuti adzabatizidwe mu Dzina la Yesu Khristu,ndipo iye analibe ngakhale zovala zirizonse kuno zoti iyeabatizidwiremo, koma ankafunabe kuti apite mulimonsemo.Ndipo Mulungu wakhala wachisomo kwa munthu ameneyo.Tangoganizani, iye wadutsitsa zaka twente pa nthawi imeneMulungu anamulonjeza iye.Mukuona?Ngati icho si chisomo!

Ndipo akadali chigonere, tsiku lina, ali ndi kulephereratukwa mtima, ndi kupweteka kwa mtima, mwaona, kuphatikizirapa izo. Ndipo ngati Mulungu akanati asamuchiritse munthuameneyo ndi kumudzutsa iye kuchokera pamenepo, nthawiyomweyo. Ndipo ine ndikukhulupirira, kuyambira pamenepo,dokotala wake anamwalira. Nkulondola uko? Ine ndamve-…Eya, kuti ngakhale dokotalayo, dokotala Wachiyuda amene—amene amamuthandiza iye, ndi zinthu, ndipo anaima mu holondipo anayankhula ndi ine zokhudza iye, iyeyo anafa.Mukuona?

Mai, ndi chochuluka bwanji, ndi chakuya bwanji chikondiChanu, OAmbuye! Chikondi Chanu ndi chachikulu bwanji!36 Tsopano, ife tiri ndi mipango ina pano imene tititiyipempherere, basi mu mphindi pang’ono chabe. Komaine ndiyankhula pang’ono za chikhulupiriro, ndipo kenakotiwona chimene Ambuye ati atsogolere, chimene ife tititichite kuchokera pamenepo kumapitirira. Chabwino, tiyenitingozisiyira izo kwa Iye, ndiyo njira yopambana. Oh, kukhaliralimodzi mumalo Ammwambamwamba!37 Ine ndinayankhula ndi ena a azimzanga, lero, ine nditathakutuluka mu Blue Boar kumeneko. Ndipo ine ndinati, “Kodi inumutsalira kuti mukhale nawo pa chiyanjano?”38 “Inde.”39 Ine ndinati, “Inu mwinamwake muyenera kuti muyendetsampaka thwelofu kapena wani koloko.” Iwo akuyembekeza kutiazikafika kwawo cha m’ma sikisi mmawa, mitunda yaitali.Kumbukirani, iwowo ndi anthu, ndipo amatopa chimodzimodzimonga ine. Kupita mpaka ku Tennessee, ndi kuzungulira, iwoazipita. Ambuye awadalitse iwo.40 Pali zinthu zochuluka kwambiri zimene ine ndikanathakunena; ine ndingotengapo nthawi yonse. Koma ine—inesindikuwonaniwonani inu pafupipafupi, ndipo ine—ine—inendimangokonda kuyankhula ndi inu,mulimonse. Komangati inesindikwanitsa kuti ndikuuzeni zonse zimene ine ndimaganiza zainu, pano,…Mukuona?

Ine ndikufuna ndiwauze abale awo. Ena a iwo atsekamatchalitchi awo.

Page 14: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

14 MAWU OLANKHULIDWA

41 M’bale Jackson, panommawa uno, anapereka kutanthauzirakokongola kuja kwa—kwa lirime losadziwika limene m’balewina anayankhula, ndipo kutsimikizira kapena kuyikirakumbuyo kuti Anali Mulungu. Kodi inu munazindikira, Iyesanati Icho sichinali cholakwika, Iye sanati Icho sichinalimomwemo; Iye anangopereka chenjezo kuti timvetsere.Mukuona? Mukuona? Chotero, M’bale Junior anali pano mmawauno, ndipo anatseka tchalitchi chake.

Ndipo ine ndamvetsedwa kuti ena a abale ochokerakumusi…matchalitchi enawo, ochokera kuno kuSellersburg.42 Ndi—ndi M’bale Ruddell, iye anali kuno mmawa uno.Ine sindikudziwa ngati iwo ali pano usikuuno kapenaayi. Chabwino, ali panonso usikuuno! Chabwino, Ambuyeakudalitseni inu, M’bale Ruddell. Ndi inu…

Ine basi sindingathe kuchifotokoza icho, basi chimene inendikuganiza. Koma mwinamwake…Chabwino, pamene ifetidzakafika ku mbali inayo, ine ndikufuna ndidzakhale pansindi inu kwa zaka teni sauzande zokha, aliyense, inu mukuona.Kenako, mwaona, ife tidzakambirana izo zonse.43 Ndipo pamene zokolola zacha, ndipo antchito ndi ochepa,tiyeni tikumbe m’menemo, mwa mwayi pakhoza kukhalawochimwa atakhala pafupi. Pakhoza kukhala winawake ameneusikuuno zikhoza kumusintha njira yonse.

Ndipo ikadakhala kuti sinthawiyo, m’mawa uno, usikuunoakhoza kutsekeraMabuku.Kumbukirani, sipadzakhalansowinawodzalowa pamenemaina amenewo awomboledwa.

Zisanatero, tsopano, aliyense amvetsere mwatcherukwenikweni ine ndisanawerenge Lemba.44 Onse amene ati adzawomboledwe, Mulungu analemba dzinalawo mu Bukhu la Moyo wa Mwanawankhosa dziko lapansilisanafike konse polengedwa. Ndi angati amene akudziwazimenezo? Limenelo ndi Lemba. [Malo opanda kanthu patepi—Mkonzi.] Ndipo wotsutsakhristu, mmasiku otsiriza,adzakhala wofanana kwambiri ndi chinthu chenichenicho,Mpingo weniweni, chirichonse chimodzimodzi basi mmeneanakhalira Yudasi, kufikira kuti izo zikanadzanyengaOsankhidwa kumene ngati kukanakhala kotheka. Nkulondolauko? Koma palibe munthu amene angadze kwa Yesupokhapokhapo Mulungu atamutumiza iye, ndipo onse ameneMulungu anawapereka kwa Iye adzabwera kwa Iye. Ndipopamene Iye akudzatenga Bukhu limenelo, dzina lomaliza…45 Mwaona, onse amum’badwowa Luther, Iye anawachotsamoiwo. Onse a mu m’badwo wa Wesley, Iye anawachotsamoiwo. Onse a mu mibadwo yosiyanasiyana, ndi m’badwowa Pentekosite, Iye amawachotsamo iwo. Iwo ali kuno,sadzaweruzidwa ndi iwo. Iwo akukwatulidwa. Ndipo kenakopamene dzina lomaliza lidzatulukira, limene linaikidwa mu

Page 15: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 15

Bukhu la Moyo wa Mwanawankhosa, amene anaphedwa mazikoa dziko lapansi asanakhazikitsidwe; pamene dzina lotsiriza ilolawomboledwa, ntchito Yake idzatsirizidwa, Iye adzabwera kutiadzawatenge amene Iye wawawombola. Zimenezo zimapangitsamtima wathu kuwukha magazi. Koma ngati zitakhala kutizikupitirira zaka chikwi mtsogolo, sipadzakhala mmodzi atiadzawomboledwe.

Ndipo palibe aliyense amene angawomboledwepokhapokhapo ngati iwo anaikidwa mu Bukhu la Moyo waMwanawankhosa maziko a dziko lapansi asanakhazikitsidwe.Kodi iwowo ndi ndani? Ine sindikudziwa. Palibe aliyense ameneakudziwa, mwaona, Mulungu yekha basi. Ine ndikudalira kutialiyense wa ife, maina athu anali pa Bukhu limenelo. Ngatilanga linali pamenepo, ine ndikutsimikiza kuti ndidzakakhalakumeneko; ngati panalibepo, ine sindidzakakhalako. Ndizozonse. Mwaona, basi, izo ziri kwa Mulungu basi. “Si iye ameneakufuna, iye amene akuthamangira, koma Mulungu ameneamawonetsa chifundo.” Mukuona?

46 Tsopano tiyeni ife tsopano tifike ku Mawu, ndi kulemekezakonse ndi kuwonamtima. Ndipo ine ndikuganiza ndicho chinthuchimodzi chimene ife tikuyenera kuchita, mwaona. Tiyeni tisiyezopusa zonsezi! Khalani olemekeza, owonamtima!

Ine ndimawona kuvomereza uko nthawizina pamene iwo…Pa televizioni, pamene iwo anali ndi msonkhano uja waBilly Graham; ndiribe kanthu kotsutsana ndi Billy Graham.Koma kunja uko mu California, munthuyo analalikira uthengawopambana usiku wotsiriza umenewo; analalikira chinthuchomwe chomwecho chimene ine ndinalalikira kuno osatikale kwambiri, pa Danieli, “Iwe wayesedwa pa muyezondipo wapezeka woperewera.” Ndi angati anaziwona zimenezo?Ambiri a inu, ine ndikuganiza.

47 Taonani, kodi inu munawawona anthu amenewoakubwera kuchokera mmipita, akutafuna chingamu, akuseka,akugunyuzana wina ndi mzake? Kumeneko si kuyenda pakatipa imfa ndi Moyo. Kumeneko sikudzimvera chisoni chifukwacha tchimo, ndi kulapa. Mukuona? Basi ndi chimene Billyamanena, “Kupanga chiganizo.” Ndipo kukhudzidwa kozizira,kwa m’maso mwa gwa, chiganizo, si zinthu, si chinthucho. Iweumayenera kuti udzimvere chisoni chifukwa cha tchimo, ndipouchokeko kwa ilo.

Ndipo Billy mwiniwake anati, “Zikutsimikizira kuti, mwasate sauzande, iwe sungapeze sate pa chaka.” Ndinanena,tsiku lina, “Kodi vuto ndi chiyani ndi New York? Ine ndinalindi msonkhano waukulu umenewo uko, ndipo chinachitikandi chiyani? Tchimo likuipirabe kuposa mmene ilo linayambalakhalirapo.”

Page 16: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

16 MAWU OLANKHULIDWA

48 Ndipo ilo lizipitirira kumaipirabe. Sikudzakhalanso ku-…kulapa kwa fuko. Fukoli lapita. Basi inuyo, anthu panokha;ndipo posachedwapa izo zidzatha, ngati izo sizinatero kale.Tsopano, inu mungolemba zimenezo, inu ana aang’ono. Taonanimpaka kuti M’bale Branham…Si M’bale Branham. Chimeneine ndanenachi ndi chabwino kapena choipa. Tchimo lifikapomaipira ipira mpaka tsiku lina miyamba idzagwirira moto,iyo idzagwera pa dziko lapansi, ndipo dziko lapansi lidzayakamoto ndi kutentha koposa. Koma, Owomboledwa sadzakhala alikuno nthawi imeneyo, iwo adzakhala atapita.49 Tsopano mu Bukhu la Marko Woyera mutu wa 11, YohaneWoyamba 4:4 ndi mu Mateyu 28:20, ine ndikufuna kutindiwerenge.50 Tsopano, poyamba, ine ndikufuna kuti ndiwerengekuchokera ku Marko Woyera, mutu wa 11, ndi ndime ya 12mpaka ya 24.

Mvetserani mwatcheru kwenikweni tsopano pamene ifetikuwerenga. Ndipo tsopano izi ziikira kumbuyo umboniwaung’ono, ndi mawu pang’ono a chirimbikitso, ndipo kenakoife tiwona chimene Ambuye atilole ife kuti tichite. Aliyensemungokhazikika ndipo mukhale mupemphero tsopano, pameneife tikuwerenga.51 Marko 11:12.

Ndipo mmawa, pamene iwo…anabwera kuchokeraku Betane, iye anali ndi njala:Ndipo powona mtengo wa mkuyu patali uli ndi

masamba, iye anabwera, ngati mwamwayi iyeangapezeko chirichonse pamenepo: ndipo pameneiye anabwera kwa iwo, iye sanapeze kalikonse komamasamba; pakuti nthawi ya mkuyu inali isanafike.Ndipo Yesu anayankha ndipo anati kwa iwo, Palibe

munthu adzadya chipatso chako kuyambira panompaka kalekale. Ndipo ophunzira ake anamva ichi.Ndipo iwo anabwera ku Yerusalemu: ndipo Yesu

anapita mu kachisi, ndipo anayamba kuwatulutsaiwo amene amagulitsa ndi kugula mu kachisi, ndipoanatembenuza magome a osinthitsa ndalama, ndimipando ya iwo amene amagulitsa nkhunda;Ndipo sanalola kuti munthu aliyense anyamule

zotengera kudutsa mu kachisi yense.Ndipo iye anaphunzitsa, nanena kwa iwo, Izo ziri…

kunalembedwa, nyumba ya Atate Anga idzatchedwaa…mwa mafuko onse nyumba ya pemphero? koma inumwaipanga iyo kukhala phanga la mbava.Ndipo alembi ndi akulu ansembe anamva ichi, ndipo

anasinkhasinkha mmene iwo akanamuwonongera iye:

Page 17: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 17

pakuti iwo—pakuti iwo amamuwopa iye, chifukwaanthu onse amazizwa pa chiphunzitso chake.Ndipo pamene madzulo anafika, iye anatuluka mu

mzindawo.Ndipo mmawa, (tsopano limenelo ndi tsiku lina),

pamene iwo amadutsa, iwo anawona mtengo wa mkuyuutauma kuchokera ku mizu.Mkati mwa maora twente foro, chozizwitsacho chinali

chitachitika, Iye atatha kunena kwa iwo, “Palibe munthuadzadya.” Panalibe, chimawoneka ngati, chachitika nthawiimeneyo; koma, pofika tsiku lotsatiralo, iwo unauma.

Ndipo Petro pokumbukira anati kwa iye, Mbuye,taonani, mtengo wa mkuyu uja umene inumunautemberera wafota.…Yesu pomuyankha iye, anati kwa iwo, Khalani ndi

chikhulupiriro mwa Mulungu.Pakuti indetu Ine ndinena ndi inu, Kuti yense amene

adzanena kwa phiri ili, Suntha iwe, ndipo ukadziponyeiwe mu nyanja; ndipo sadzakaika mu mtima mwake,koma adzakhulupirira kuti zinthu zimenezo zimene iyewazinena zidzachitika; iye adzakhala ndi chirichonsechimene iye wachinena.Chotero Ine ndinena ndi inu, Zinthu zirizonse

zimene inu muzikhumba, pamene inu mupemphera,mukhulupirire kuti inu mwalandira izo, ndipo inumudzakhala nazo izo.Ndipo pamene inu muima ndi kupemphera,

khululukirani, ngati inu muli ndi mangawa ndialiyense: kuti Atate wanunso amene ali kumwambaakathe kukukhululukirani mphulupulu zanu.Koma ngati inu simukhululukira, Atate wanunso

amene ali kumwamba sadzakukhululukiranimphulupulu zanu. (Izo ziri pa mangawa.)

52 Tsopano ine ndikufuna kuti ndiwerenge Yohane Woyamba4:4.

Inu ndi a Mulungu, ana aang’ono, ndipomwawagonjetsa iwo: chifukwa…(mvetseranimwatcheru)…wamkulu ali iye amene ali mwa inu,kuposa iye amene ali mdziko.

53 Ine ndiwerengenso ichi kachiwiri tsopano.Inu ndi a Mulungu, ana aang’ono, ndipo

mwawagonjetsa iwo: (akukamba za wotsutsakhristu),chifukwa wamkulu ali iye amene ali mwa inu, kuposaiye amene ali mdziko.

Page 18: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

18 MAWU OLANKHULIDWA

Alowam’malo awiri, mwaona, “iye,” mlowam’malo wamunthu; “iye” amene ali mdziko, ndi “Iye” amene ali mwa inu.“Iye amene ali mwa inu ndi wamkulu kuposa iye amene alimdziko.”54 Tsopano, ndipo a—a mutu wa 28 wa Mateyu Woyera, ndindime ya 20.

Kuwaphunzitsa iwo kuti asunge zinthu zonse zimeneIne ndinakulamulirani inu:…taonani, Ine ndiri ndiinu nthawizonse, ngakhale mpaka kumapeto a dzikolapansi.

55 Tsopano mutu kuchokera pamenepo, usikuuno, inendikufuna kuti ndigwiritse ntchito ichi ngati mutu: Iye AmeneAli Mwa Inu. Ndipo pa ichi ine ndikufuna kuti ndiwumbepochikhulupiriro, ndithudi, cha msonkhano wa pemphero. Ndipomwamsanga basi…56 Tsopano, izo ziri monga ine ndakuuzirani inu, inendimakonda kukudziwitsani inu zinthu zimene zachitika.Ndipo ine kawirikawiri ndimadikirira mpaka ine ndifike ku—ku tchalitchi kuno, kuti ndidzanene zochitikazo. Ndiyeno ngatiena akukonda kuti akazimvetsere izo, iwo atha kukazimvera izokudzera pa matepi. Koma ine ndimadikirira mpaka ine ndifikekuno.

Ndipo pali, pafupifupi, pa chochitika ichi chimene inenditi ndikuuzeni inu pompano, pali amuna angapo pano ameneali mboni za izi, abale Achikhristu. M’modzi amene analipo,anali M’bale Banks Wood. Wina amene analipo, anali M’baleDavid Wood. Wina, amene alipo pano, anali M’bale Evans ndimwana wake, Ronald. Winanso amene analipo, ndi dikoni wathuwochirimika, M’bale Wheeler. Ndipo wina, analipo, anali M’baleMann. Kodi M’bale Mann ali pano, wochokera ku New Albany?Mlaliki wa Methodisti yemwe ndinamubatiza mu Dzina la YesuKhristu, posachedwapa, iye anali kumeneko, nayenso, pameneichi chimachitika.57 Zakhala kwa kanthawi, kwa zaka pang’ono, mmeneine ndakhalira ndi kulemedwa kwakukulu pa chifuwachanga mwakuti ine…mu mtima mwanga. Ndimazimvereramwa ine ngati kuti ine ndachita chinachake cholakwika.Ndipo ndinafufuza moyo wanga, mobwereza bwereza ndimobwereza, kuti ndiwone chimene chalakwika. “Ambuye,ngati—ngati ine ndachita chirichonse cholakwika, ndiyeInu mungochiulula icho kwa ine, chimene chalakwikacho,ndipo ine ndipita ndi kukachikonza icho.” Koma panalibechimene chimaululidwa kwa ine. Ine ndimatha kunena kuti,“Kodi ine ndinamupweteka aliyense? Kodi ine ndinasiyachinachake osachichita? Kodi ine…kodi ine ndikuwerengamokwanira? Kodi ine ndikupemphera mokwanira?” Ndipoine ndimawerenga ndi kupemphera. Ndipo—ine ndimati—ine

Page 19: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 19

ndimati, “Ndiululireni ine chimenecho. Kodi ine ndamupwetekaaliyense, kwinakwake? Ngati ine ndatero, ine ndikachikonzaicho. Ingondisonyezani ine; ine sindikufuna kulemedwa uku.”Ndipo kwa zaka faifi zapitazi, chichokereni ine ku ntchito,pakhala pali kulemedwa uku kukulendewera mu mtimamwanga.58 Ine ndapita ku mapiri. Ine ndapita mmphepete mwa nyanja.Ine ndapita kulikonseko, ndipo ndapemphera ndi kupempherandi kupemphera, ndipo icho sichimachoka basi. Ndipo inendinaganizira za chirichonse, ngati ine ndachita chirichonse.Koma icho, apobe, icho sichimachoka; ine ndinangokhala mumsinga, basi.

Ndipo ndi zachilendo kwambiri kuti ichi chinachotsedwapa nthawi imene Uthenga uwu umabwera, mwaona, wa mmawauno. Tsopano, kodi anali Mulungu kuti amasungira chifukwacha ichi? Ine sindikudziwa. Mwaona, ine…Zinthu izi zonsezinali mmalingaliro anga. Inu mutha kulingalira zimenezimakhala mu mtima wa munthu pamene iwe ukupirira ndi izo,mwaona, kumaganizira za zimene zikuchitika; ndi, kumadziwa,kuti uwauze anthu, kumadziwa kuti ena apendekekeramolakwika, ndipo ena apita njira iyi, ndi njira iyo. Ndipo iwenkumadziwa mmene izo ziliri. Ndipo ena akhulupirira, ndipoena satero. Ndipo, koma ndizo zimene iwe uyenera kupiriranazo.59 Iwe unganene bwanji izo popanda kupweteka? Iwe unganenebwanji izi, kuti izi zichitika? Iwe unganene bwanji izi, kutiuwasonyeze anthu kuti iwe siuli—iwe sukuwanena iwo, kutiiwe umawakonda iwo? Iwe ungakhale bwanji wosamalitsa ndiwochirimika, ndipo komabe nkukhala wokonda? Ndipo, oh,kodi iwe uchipereka motani icho? Ndiyeno tsoka kwa inengati ine sindichipereka icho! Mukuona? Ndipo ndi zimenezotu.Mukuona? Nzosadabwitsa, izo zimakupangitsa iwe kukhalawamanjenje ndi wosweka.60 Ine ndinali nditatsika kuchokera ku—kuchokera…ndinabwera kuchokera ku Arizona, kuti ndidzakumane ndi gulula abale kuno, amene amapita kokasaka ndi ine ku Colorado,chaka ndi chaka.

Tsopano, anthu ena akhala akudabwa, “Chifukwa chiyaniinumumapita kokasaka? Chimakupangitsani inu ndi chiyani?”

Mwaona, pano, inu mukudzadzitsa, ine ndikukhuthula;kumeneko, ine ndimakhala ndikudzadzitsa, kuti inendidzakhuthule. Mukuona? Tsopano, ine sindimangopita kutindikangowombera nyama. Bwanji, anthu, aliyense pano ameneamapita ndi ine, amadziwa kuti ine ndimadutsamazana a nyamandipo osazikhudza nkomwe izo. Ine sinditero.61 Tsopano, kuno osati kale kwambiri, ine ndinayambakuwombera nyama za a Christian businessmen, pamene iwo

Page 20: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

20 MAWU OLANKHULIDWA

apita nawo ndipo amati, “Billy, ndipezere ine nkhudzi, ndipezereine ng’ombe, ndipezere ine mphoyo, ndipezere ine iyi, kapenaiyo, imzakeyo.” Ine ndimapita ndi kukangowombera nyama,kuyambira kumanja ndi kumanzere. Ambuye amandithandizaine mwakuti ndimaziwona ndipo ndimapeza nyama, ndikuwombera kwabwino ndithu, ndi kuziwombera izo. Ndipo—ndipo iwo amangokhala mozungulira ndi kumakambirana zageni zawo.62 Kenako Ambuye anadzandiuza ine kuti ndisamachitensoizo. Ndipo ine—ine ndinamverera moipa za izo, chotero inendinamulonjeza Iye kuti ine sindimachitanso izo. Ayi. Inendinati, “Ngati zikhala zofunikira ndipo winawake akuisowaiyo, ine ndizikachita izo. Koma ngati iwo sakuzisowa izo,ine sindimachita izo.” Basi amuna amenewo, iwo ali ndindalama zambiri zoti akhoza kugula nyama ndi zinthu. Choteronchifukwa chiyani kuti ine ndizichita zimenezo? Isiyeni nyamayoikhale moyo ngati inu simukaigwiritsa ntchito iyo.63 Chotero ine ndimangopita kuti ndikakhaleko ndekha.Ndipo munthu aliyense, amene amapita kukasaka ndi ine,amadziwa kuti ine sindisaka ndi aliyense. Ine ndimapita kwandekha, kuti ndikakhale ndekha. Ine ndimapita nawo iwo, kutitizikakhala ndi chiyanjano usiku, kukaima titazungulira ndikumapemphera, ndi zina zotero.

Koma kunali azitumiki ena ambiri kumeneko. Uko kunali,uko mmapiri chaka chino, kunali M’bale wathu Palmer.Ine ndikukhulupirira ine ndinamuwona iye kwinakwakenthawi ina…Ndi uyu apa, wakhala apayu, M’bale Palmer.Ndipo M’bale Bob Lambert, iye anali pano mmawa uno, inendinamumva iye akufuula penapake. Ine ndikuganiza iyeakadali pano. Ndiyeno apo panali m’bale…anyamata awiria Martin, ine ndikuganiza iwo ali pano. Kodi iwo alipo,anyamata a Martin? M’bale, M’bale Martin. Inu munandiimbiraine tsiku lina, zimenezo zinali zabwino. Mnyamata ameneyoanachiritsidwa, m’bale mtumiki uja.64 Kodi iwe uli pano, iye amene ine ndinamupempherera, pafoni, tsiku lina? Ine ndaiwala dzina lake, wochokera kuArkansasuko. Mkazi wake anandiimbira ine; bamboyo anali atatupiratukumbaliku, ndi kutentha kwa thupi, akufa. Bambo yemweyoyemwe anaitanidwa, kumusi uko—ku Little Rock, kapenamsonkhanowa kuHot Springs, atakhalamumsonkhano.

Ndipo ndi mnyamata wowoneka bwino. Ngati iye ali pano,ine ndikuganiza iye sadzuka tsopano, nkomwe. Koma inendaiwala dzina lake. Ine ndikulephera kuganizira dzina lake.[Winawake akuti, “M’bale Blair.”—Mkonzi.] Blair, M’bale Blair.Winawake…

Chabwino, tsopano, titakhalamumsonkhano kuLittle Rock,ndi angati amene anapita, ine ndikutanthauza, ku Hot Springs,

Page 21: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 21

ndi angati amene anali pa msonkhanowo? Ndipo Mzimu Woyeraunamuitana mnyamata wamng’ono ameneyo ndipo unamuuzaiye kuti mdierekezi amayesetsa kuti amupangitse iye kutiandikane ine, kuti anene kuti ine ndine “mneneri wabodza.”Ndipo munthuyo anachitira umboni kuti izo zinali zoona. Inumukuona zimene mdierekezi amachita? Munthuyo samapitakwa madokotala. Iye sakhulupirira kupita kwa madokotala.Koma Satana amadziwa kuti nthenda iyi imukantha iye,ndipo iye akanatha kumupha iye pomwepo. Mukuona? Choteroiye amayesetsa kuti amupangitse iye kuti andikane ine.Ndipo Mzimu Woyera, mwa chisomo, unamuitana iye ndipounamuuza iye kuti asachite zimenezo; munthuyo, pokhalamlendo, unamuitana iye kuti asachite zimenezo.65 Ndipo usiku wina, mkazi wake anandiimbira ine ndipoanati, “M’bale Branham, ine ndikukhulupirira kuti iyeakufa.” Anati, “Iye ali—iye watupikana. Ndipo, watenthathupi, iye wazungulira mutu, pafupifupi.” Ndipo anati,“Chinthu chomalizira chimene iye wanena, ‘Muimbileni M’baleBranham.’”

Ine ndinati, “Kodi inu muli ndi chirichonse, mchikwamamwanu muli mpango?”

“Ayi.” Ine ndinali ku Tucson; iye anali kuArkansas.Ndipo ine ndinati, “Muli ndi chirichonse?”Iye anati, ine ndikukhulupirira, “sikafu” yake.Ine ndinati, “Tsopano muike dzanja lanu pa sikafu, ndipo

mugwire choyankhulira foni mu dzanja linalo.” Ndipo inendinapemphera ndipo ndinamufunsa Mulungu kuti amuchitirechifundo ndipo amukanize mdani ameneyo.66 Ndipo iye anapita ndipo anakaika sikafuyo pa munthuyo.Ndipommawawotsatira, iye anandiimbira ine.

Tsopano, mu maora twente-foro, kapena ochepera paamenewo.67 M’bale wathu wofunika, ine sindinamuwone iye usikuunopanobe, M’bale Roy Roberson. Ndipo nthawiina, inumukudziwa, M’bale Roy anali ngati wakunkhondo. Ngatiiye ali pano, ine—ine ndikuyembekeza iye akumvetsetsa,chifukwa ine—ine—ine sindikutsutsa izo. Koma chirichonsechimakhala mosamalitsa, iye anali wamkulu ku Nkhondo,inu mukudziwa, ndipo iwe umayenera kukhala wozoloweramomwe ukuchitira ndi anthu monga mmene iwo amachitira kuNkhondo. “Chabwino, zinthu zauzimu izi kwa munthu wina,”osati iye! Koma Ambuye anamupulumutsa iye. Iye akanakhalaatafa; iwo anakamuika kumeneko kuti wafa, kwa nthawiyaitali. Ambuye anamuchiritsa iye; iye wakhala akutsatirakuchokera nthawi imeneyo. Koma zinthu zauzimu zonse izi, iyesamazidziwa izo, ndi masomphenya.

Page 22: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

22 MAWU OLANKHULIDWA

68 Ndipo kuno osati kale kwambiri, ambiri mukudziwamasomphenya amene anaperekedwa kwa M’bale Roy ngakhaleine ndisanapite nkomwe kumeneko, okhudzana ndi iye kutianandiwona ine nditaimirira pa phiri kumeneko, mu Kuwalakuja, ndipo Liwu likubwera kuchokera kwa ine. Chimenechochinachotsa kukaikira konse kwaM’bale Roy.69 Ndipo usiku wina iye anakanthidwa mu malo amenewokufikira kuti iye anadwala kwambiri, ndipo anatentha thupikwambiri, ndi zinthu. Ndipo adokotala anamupatsa iyemankhwala, chirichonse, ndiyeno izo sizinachite ubwinouliwonse. Ndipo iye mpaka anafika pa malo akuti samathangakhale kudzisunthapo yekha. Miyendo yake ndi zinthu zinali,ngati, zapuwala.70 Ndipo m’bale wosauka wamng’onoyo anawomberedwapomzidutswa, ndi tizitsulo ta m’bomba la eyite-eyiti, Germaneyite-eyiti. Ndipo ilo—ilo linali basi…Ndipo ine ndikuganizagulu lake lonse linaphedwa, koma iyeyo, ndipo pamenepo iyeanawomberedwa mzidutswa.71 Ndipo inu mukudziwa chimene chinachitika? Inendinamuuza mkazi wake wochirimika, Mlongo Roberson,kuti…Iye anati…Ine ndinati, “Muli ndi chirichonsepamenepo?”72 Iye anati, “Ine ndiri ndi mpango umene inumunawupempherera.”73 “Pitani mukautenge iwo.” Ndipo ine ndinali ku Tucson,ndipo anaika dzanja lake pa iwo, ndipo tinapemphera ndikuchidzudzula, ndipo ndinati, “MlongoRoberson, izo zitha.”74 Basi Chinachake chandiuza ine pamenepo, “Izo zitha. Uneneizo!” Ndipo mkatikati mwa theka la ora, kutentha kwathupikokunali kutatha; iye anali mu khitchini, akusakasaka chinachakechoti adye. Mukuona? Mukuona?75 Chimene ine ndikuyesera kuti ndinene, “Musataye konsechidaliro chanu.” Musamulole Satana azikuuzani zoyipa zaine; chifukwa, ziripo zambiri. Koma inu musunge chidalirochimenecho; chifukwa, ngati inu simutero, izo sizichitika.Musamayang’ane pa ine, ngati munthu; ndine munthu, ndinewodzadza ndi zolakwitsa. Koma muziyang’ana kwa zimene inendikunena za Iye. Ndi Iyeyo. Iye ndi Ameneyo.76 Pamene ife tinali ku Colorado, mwaona, pamene ifetinali pamwamba kumeneko, ife tinabwererako. Ndipo kunalikuli kowuma kwenikweni. Nyama zimasowa. M’bale Wheeler,Ambuye anamudalitsa iye ndipo anamupatsa iye a—nyamayabwino, ndipo ife tinali wosangalala kwambiri ndi chimenecho.Inali nthawi yoyamba imene iye anakhalapo m’nkhalangokukasaka, ndipo Ambuye anamudalitsa iye. Ndiyeno ine ndinalinditawombera nyama yaikulu imene ine ndinakhala ndikuifunakwa zaka twente, ndakhala ndikuifuna iyo, M’bale Banks ndi

Page 23: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 23

ine takhala tikuifuna iyo kwa nthawi yayitali. Ndipo pameneine ndinatero…Kukawombera mfuti yanga ku dera lotenthailo, nditaibweretsa iyo kozizira, zinafufumitsa chithunthucho,ngakhale icho chinali cha galasi. Ndipo iyo inakawomberaiyo pambali mainchesi angapo, ndipo inakawombera nyamayo,itaima pakati pa mitengo, pamene iyo siimayenera kuiwomberaiyo; kutsikirako mmusi, zimene ikanapha mwabwino nyamayomumphindi. Koma iyo inakawombera iyo mmwamba kwambiri,iyo, iyo inalumpha,mpaka iyo inakagwamonga choncho.77 Ndipo Billy anali ndi ine, ndipo iye anati, “Icho chamupezaiye.” Ndipo ine ndimaganiza icho chatero, inenso; koma pameneife tinadzapita pamenepo, izo sizinali chomwecho. Iye anati,“Inu munawombera mtengo.” Ine ndinayang’ana mokweza ndimotsitsa, panalibe chizindikiro pa mtengopo. Ndiyeno inendinapita kumakaifufuza iyo.

Ndipo kenako panadzabwera chizindikiro cha chenjezo.Panali ndithudi amuna handiredi, pamwamba pathu pomwe.Ndipo M’bale Palmer ndi iwo ndi mboni a zimenezo. NdipoM’bale Evans, uko nkulondola, iye anali kumeneko; M’baleWelch Evans ndi mnyamata wawo, Ronnie. Ine ndikukhulupiriraine ndinawatchula iwo, kanthawi kapitako. Ndipo gululalikulu la amuna linali litakwera pamtunda pathu, kumeneiwo amakutcha msasa wa ng’ombe kumeneko, kumeneanyamata olishya ng’ombe amakhalako ndi kumakwera,amazilekanitsa ng’ombezo. Ine ndinkakonda kukhala mu msasaumenewo inemwini ndi kumalishya ng’ombe zimenezo ndikumazilekanitsa izo.78 Ndiyeno, chotero, mmenemo, munali pafupifupi amunahandiredi. Koma aliyense amadziwa, ku dera limenelo,pamene nkuntho ulengezedwa, iwe umayenera kuti uchokeretupomwepo. Nchifukwa chake M’bale Palmer ndi iwo anachokamolawirira, chifukwa iwo anangokhala ndi liwiro litatu mugalimoto yawo, ndipo iwo amayenera kuti achokeko kumeneko;chifukwa, nyengo, iwe ukakhala kumeneko, ndipo iwe ukhozakukhalako kwa masabata. Chotero iwo anati, “Kuli nkunthoumene ukubwera,” kulengeza za nyengo, mapepala, wailesi.Mulu ndi mulu, pafupifupi chirichonse kuyambira mmwambakozungulira kumeneko chinachokako. Iwo anali atapita, nthawiyomweyo, chifukwa iwo amadziwa momwe angatulukirekumeneko.79 Koma abale anga anali ndi chilolezo cha agwape awiri,ndipo iwo—iwo samafuna kuti azipita. Kotero ine—ine ndinati,“Chabwino, ife titsalira.” Koma ine ndinali ndi msonkhanoumene ukubwera, mu pafupifupi masiku sikisi, ndipo inendimayenera kuti ndibwerere ku Tucson.80 Kotero, mkazi wanga wachichepere, ine…ife takhalatitakwatirana kwa zaka twente-thuu. Ndipo zaka twente, pa

Page 24: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

24 MAWU OLANKHULIDWA

chikondwerero chathu, ine ndakhala ndiri kumeneko nthawiiliyonse; zimangochitika kuti ndimakhala ndiri kumeneko.Chotero ine—ine ndiri ndi malo aang’ono amene ine nthawizonsendimayenderako ndi kukapemphera, ndipo iwo amawonekangati malo amene ine ndinamutengerako iye.81 Inu mukudziwa, ine ndinapanga ngati kanthu kakang’ono,inu mukudziwa, ine ndinalibe ndalama zokwanira kuti ndikhalendi ulendo wokasaka ndi wokakhala kwa tokha wanga,chotero ine—ine—ndinakhala ngati ndinamutengera mkaziwanga pa ulendo wokasaka ngati wokakhala kwa tokha.Chotero ife tinali mu New York, ndipo ine ndikukumbukirandikumuthandizira iye kulumpha zipika ndi zinthu, tikupita kumaloko. Ndipo ine ndiri ndi kamalo kakang’ono kumeneko, inenthawizonse ndimaganizira za iye pamene ine ndipita kumenekopa chikondwerero chathu. Okutobala twente-firii ndi pameneamatsegula nyengo yake kumeneko. Ndipo, zaka twente, inendakhala ndisakukhala pakhomo, nthawizonse kumeneko.82 Chotero tsiku limenelo linali tsiku la chikondwerero chathu.Ndipo M’bale Mann…Ine ndinati, “Tsopano ngati abaleinu…” Ine ndinati, kwa moto, mmawa umenewo, “Tsopanongati…” Usiku umenewo, kani. “Ngati inu nonse mukufunakutsalira tsopano, mukumbukire, ife titha kukhala kuno kwamwezi.” Chifukwa ine ndawonapo mapazi twente a chisanuchikugwa basi mu kuchezera pang’ono, kwa usiku. Basi,iwe ukapita uko, ndipo kumangokhala kowuma basi ndikwabwinobwino; ndipo mmawa wotsatirawo, chisanu nkukhalachitazama chonchi, pamwamba, mwinamwake pamwambapa hema wanu. Kotero ndiye ine ndinati…Ndiyeno inunkukhala kumeneko kufikira icho chitasungunuka. Choteroinu muli pafupifupi mamailosi fifitini mpaka twente kutalimu chipululu. Ndipo kotero ndiye ine ndinati…Ndipo ngatizifika pa ngozi, ndithudi, iwo amatumizako ma helikopitandipo amakakuchotsaniko inu. Koma, kawirikawiri, iwo basi…palibe amafa, iwo amangoyenera kuti adikirire kumeneko.83 Chotero aliyense amangochokako mwamsanga pamene iwoamva kulengeza za nyengo kumeneko, kulosera, kani. Koteroife tinali tiri kutali kumeneko, ndipo ine ndinati, “Tsopano inumupange chiganizo chanu. Ngati inumukufuna kuti mutsale, inendikhala kuno kuti ndizisaka ndi inu, ndipo ine ndimuimbiramkazi wanga ndi kumuuza iye, ‘Chikondwerero Chosangalala!’”Koma ine ndinati, “Ndiye, potero, ine nditeronso, ine ndi, ifeti…Ife tikapeza zogula zina, chifukwa ife tikhoza kukhalakuno.” Ife buledi anali atatithera nthawi imeneyo. Ndipoine sindimafunanso kuwona zikokoto kwa nthawi yaitali,mapanikeke amenewo! Chotero, ndiye, ine ndinakhala ndikudyaiwo mu Canada, kwa pafupifupi masiku twente-wani, ndipondithudi ine ndinali nditakhuta zinthu zimenezo. Ndipo koteroine ndinkafuna kuti ndikapeze buledi wina.

Page 25: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 25

84 Chotero iwo anangonena kuti iwo amafuna kuti atsalire.Chotero uko kunalibe chirichonse choti nkuchita…kutititsalire. KomaM’bale Mann ndi ine tinachokako, ndipo tinapitauko ndipo timakapeza zoti tikagule. Ndipo ine ndinamuimbiramkazi wanga, ndipo foni siimayankhidwa. Panalibe ameneamayankha; chotero ine ndinadikirira pafupifupi ora mpakaife tinatsiriza kugula zogulagula, ndinabwereranso, kukaimba,iye sanayankhe. Ndipo ine ndinachita kumuimbira MlongoEvans.

Ine ndikukhulupirira Mlongo Evans ali pano. Ndipo inendinamuuza…Eya,M’bale Evans,Mlongo Evans ali pano.85 Chotero ine ndinamuimbira Mlongo Evans, mmalomwa M’bale Evans, ndipo ndinamuuza iye. Iye anati, “inendimuimbira Mlongo Branham ndipo ndimuuza iye.” A“Chikondwerero Chachisangalalo,” ndithudi, inu mukudziwa.Chotero, koma iye anali atapita kokagula zinthu, kuti akapezezogulagula zapakhomo za ana.

Ndipo kenako ife tinabwerako. Ndipo mmawa wotsatirawo,mu mlengalenga munali chiyani koma mitambo. Inali isanagwemvula kumeneko kugwa kwa masamba konse, ndipo kunalikutauma kwenikweni. Ndipo iwo anachita kutalikitsa nyengoyosakayo, masiku pang’ono owonjezera, pa chifukwa chakuumako.86 Chabwino, ine ndinati kwa abale mmawa umenewo,“Tsopano, dontho loyamba la mvula likayamba kugwa, chisanuchoyamba, chibumwa choyamba, chirichonsecho,muthamangireku msasa mwamphamvu mmene inu mungathere, chifukwamma miniti fifitini inu simudzatha kuliwona dzanja lanupatsogolo panu. Mukuona? Ndipo iyo idzingopotokola ndikumawomba, ndipo ine sindikusamala kaya inu mukulidziwabwino chotani derali, inu—inu mudzakhala pomwepo, ndipomudzafa. Chifukwa nthawizina iwe umalephera kupumankomwe, zibumwa zikuwomba chotero, ndipo, iwe umaferapomwepo.” Ndipo ine ndinati, “Mwamsanga iyo ikayambandi zibumwa zimenezo, inu muzinyamuka wa ku msasamwamphamvu basi mmene inu mungathere, ine sindikusamalakumene inu muli.”87 Chabwino, ine ndinati, “Mudzapite kuntunda kunondipo mukakhale mu madwale awa, ndipo ine ndidzakwerapamwamba ndipo ndikagudubuza miyala pa phiripo, ndizina zotero, kuti ndikawopsyeze agwapewo pamwambapo, ndikuwathamangitsira iwo kumusi, inu mudzatengepo imene inumukuifuna.”88 Chotero ine ndinayamba kukwera chokweza, ndipopafupifupi nthawi imene ine ndinakafika pamene ifetimapatchula, “pachikweza,” kamalo kakang’ono kumenekokamene ine nthawizonse ndimawolokera popita ku malo

Page 26: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

26 MAWU OLANKHULIDWA

otchedwa “Quaker Knob,” ku Continental Divide kumeneko,pamwamba pomwe. Ndipo pamene ine ndinafika pafupifupipachikweza chaching’ono ichi, iyi…mitambo inali ikuyambakumada ndi kumada. Kunalibe galimoto inatsalirako,tinangotsala ife pamwamba apo, kutali basi…ndi wolishyang’ombe mu msasa. Chotero zinafika—zinafika poipiraipira.Chotero, mu maminiti pang’ono, inayamba kuvumba mvula.Chabwino, ine ndinatenga mfuti yanga ndipo ndinadzaiyikaiyo pansi pa chikhoti changa, kuwopetsa namulondolawake kuti asafuke, ndipo—ndi thunthulo kuti lisanyowe;mwina nkugundana ndi chimbalangondo kapena chinachake,chikubwerera, chotero ine—ine ndinagwira namulondola wakemonga choncho ndipo ndinakakhala pansi pa mtengo, pang’onochabe. Ndipo ndinakhala pamenepo, ndi kumapemphera. Inendinati, “Ambuye Mulungu, Ndinu Yehova Wamkulu, ndipo inendimakukondani Inu.”89 Ndi zondichitikira zingati zimene ine ndakhala nazo! Inendinaloza kwa abale, M’bale Palmer ndi iwo, malo ake. Kumene,mphungu, inu mukudziwa, ine ndinaiwona iyo ikudzuka tsikulimenelo, inu mukudziwa, ndi momwe…Malo amene izo zonsezinachitikirako kumeneko. Ndi chinthu chokhudzamtima kwaine, kumeneko. Ine ndakhalapo nazo zondichitikira zazikuluzambiri ndi Ambuye wanga, pamwamba pamapiri amenewo.Chotero iwe sungathe kupita kumeneko popanda kumuwona Iye;Iye amangokhala paliponse.90 Chotero ndiye pamene ine—ine nditakhala pamenepo,ndiye chisanu chinayamba, ndipo mphepo ikupotokola, mongachoncho. Ndipo ine ndinati, “Chabwino, ine ndikudziwa njirayotsikira, koma ine ndibwino kuti ndichokeko kuno pompano.”Chotero ine ndinati…91 Izo zimawoneka mmusi, ndipo ine sindimatha nkomwekuti ndiwone pansipo; mitambo imeneyo ikungozungulirandi kumapotokola, ndipo chisanu chikuwomba. Ndipo zinalipamenepo, nkuntho! Kulengeza zanyengo kwa masiku angapo,“Nkuntho waukulu ukubwera!”92 M’bale Tom ali pano. M’bale Tom Simpson, akubwera kunokuchokera ku Canada, anamva akulengeza zanyengo, ndipoiye analangizidwa kuti asadutse kudzera mbali imeneyo yadziko, chifukwa kulengeza kwa zanyengo uku kunati, “Kukhalankuntho.” Kodi inu muli pati, M’bale Tom? Ine ndikuganizachomwecho, eya, pomwe pano. Ndipo iye…Nkuntho unaliukubwera! Aliyense anali atawukonzekera iwo.93 Chabwino, ine ndinabwezeretsa mfuti yanga pansi pamalaya anga, monga chonchi, malaya anga ofiira, ndinayambakuyenda kutsika phiri. Ndipo pamene ine ndinayamba, ndinalinditachoka theka la mailosi kuchokera pa chikwezacho;ndipo, oh, mai, madontho aakulu a chisanu, monga choncho,

Page 27: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 27

ndipo mphepo ikukupiza, pa phiri limenelo, ndi kumawomba.Ine sindimathanso kuwona mmusi nkomwe. Ine ndimathakuwona pafupifupi mapazi twente kutsogolo kwanga, kapenasate. Ndipo ine ndinadziwa kutsika pang’ono, chimene ifetimachitcha, “kubwerera chammbuyo pang’ono kwa nguluwe,”chitunda pang’ono, kenako ndinatsikira ku mtsinje, ndiponditatero ine ndinadziwa kutsatira ka mtsinjeko, ndi kumenendimayenera kuti ndizipita, ngati zitafika poipa kwenikweni.94 Ndipo chotero ndiye ine ndinayamba kumatsika, ndipondinafika pafupifupi theka la njirayo kumusi uko, ndipoChinachake chinati kwa ine, momveka bwino basi monga inumukundimvera ine, “Ima, ndipo ubwerere!”95 Chabwino, ine ndinaganiza, “Kodi ine ndimaganizachiyani? Mwinamwake ndi malingaliro anga chabe.” Ndipo inesindinathe kuti ndiponde phazi lina patsogolo.96 David anali atandikonzera ine sangweji mmawa umenewo,ndipo ine ndikuganiza iye amayesera kuti andikonzere inechifukwa chakuti ndinawakonzera abambo ake ina, nthawi ina,ya anyezi ndi uchi, ndizo zonse zimene ife tinadya. Choteroiye anandikonzera ine sangweji yokhala ndi zinthu zambirimkati mwake ndi, oh, ine sindikudziwa chimene izo zonsezinali, atazikulunga mmenemo! Ndipo ine ndinali nditaiyikaiyo mmalaya mwanga, ndipo iyo inali itanyowa mmalayaangawo. Ine ndinaganiza, “ine ndingoima ndidye izi, ndipomwinamwake ine ndi…Izo zikhala bwino ndikatero.” Choteroine ndinatulutsa sangwejiyo, cha m’ma teni koloko, ndipo inendinayamba kudya sangwejiyo. Ndipo pamene ine ndimadyasangwejiyo, ine ndinaganiza, “Tsopano ine ndikhala bwino.”

Ndipo ine ndinayamba kumapitirira, koma Chinachakechinati, “Ubwerere kumene iwe ukuchokera!”97 “Ndibwerere kudutsa nkunthowo, theka la mailosi kapenakuposerapo ndibwerere pamwamba pa phiri, ndilowe munkhalango ya mdima imeneyo?” Kumene, iwe sungathepamenepo kuwona utali wa pamene pali limbapo! Koma inendikuyamba kukalamba, ndipo ine ndakhala ndiri Mkhristutsopano kwa zaka sate-firii; ndipo ine ndikudziwa, ziribe kanthukaya ndi chiyani, kaya zikuwoneka zopusa bwanji, usamale zaAmbuye, uchite chimene Ambuye akunena.98 Ndipo ine ndinapotoloka ndipo ndinabwererapachikwezapo, ndikupaza mnjiramo pobwerera. Oh, zibumwazikuyamba kumalimba ndi kumalimba; kukuyamba kumachitamdima ndimdima. Ndipo ine ndinakhala pansi pamenepo, ndipondinangokoleka chikhoti changa m’mwamba monga chonchi,kapena malaya anga nditaphimba namulondolayo aponso;ndinakhala pansi. Ine ndinaganiza, “Kodi ine ndikuchita chiyanikuno?Nchifukwa chiyani ine ndabwerera pamwamba pano?”

Page 28: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

28 MAWU OLANKHULIDWA

99 Ndipo ine ndinangodikirira maminiti pang’ono. Ndipo inendinayamba kukweranso, ndipo momveka bwino basi mmeneine ndikanafunira kumvera, Liwu linati, “Ine ndine Mlengiwa miyamba ndi dziko lapansi! Ine ndimapanga mphepo ndimvula.” Ine ndinavula chipewa changa.100 Ine ndinati, “YehovaWamkulu, kodi ameneyo ndi Inu?”101 Iye anati, “Ine ndinali Iye Amene anapangitsa mphepo kutiisiye pa nyanja. Ine ndinali Iye Amene anapangitsamafunde kutiasiye. Ine ndinalenga miyamba ndi dziko lapansi. Kodi sindinaliIne Amene ndinakuuza iwe kuti uyankhule kwa, agologolo aja,ndipo iwo anakhalapo? Ine ndineMulungu.”102 Tsopano, pamene liwu liyankhula kwa iwe, uziyang’anaLemba. Ngati izo siziri Mwamalemba, iwe uzisiye izo zokha;ine sindikusamala kaya izo zikumveka mwabwino bwanji, inumukhale kutali ndi izo.103 Ine ndinati, “Inde, Ambuye.”104 Iye anati, “Yankhula kwa mphepo zimenezo ndi nkunthouwo, ndipo izo zichoka.” Tsopano, Baibulo ili liri patsogolopanga, limene moyo wanga uli mwa Ilo.105 Ine ndinadzuka, ine ndinati, “ine sindikukaikira Liwu Lanu,Ambuye.” Ine ndinati, “Mitambo, chisanu, mvula, zibumwa, inendikukaniza kubwera kwanu. Mu Dzina la Yesu Khristu, pitaniku malo anu! Ine ndikunena kuti dzuwa libwere pompano ndipoliwale kwa masiku anayi, kufikira ulendo wathu wosaka utathandipo ine ndinyamuke ndi abale angawa.”106 Iyo imangokhuthuka, imangopita, “Whuuuushi,” mongachoncho. Ndipo inayamba kupita, kumapita, “Whuushi,” kenakoiyo inapita, “whii, whii, whii,whee.” Inasiya!107 Ine ndinaima mwabata kwenikweni. Abale anga alikuntunda uko, ndipo amadabwa kuti kukuchitika chiyani.Ndipo zibumwa, mvula zinasiya. Kunadzabwera mphepoikukupiza kumatsikira kudutsa mmapiriwo, inakungunuliram’mwamba mitambo, ndipo wina unapita njira iyi; kummawa,kumpoto, kumadzulo ndi kummwera. Ndipo, mu maminitipang’ono, dzuwa linali likuwala mwabwino ndi mofunda. Izonzoona! Mulungu akudziwa kuti izo nzoona!108 Ine ndinangoima pamenepo, ndi kumangoyang’anayang’ana;nditavula chipewa changa, ndikuyang’ana. Ine…Inumukuti…ine ndinachita dzanzi, paliponse.109 Ine ndinaganiza, “Mulungu kumene wa Chirengedwe, zonseziri mmanjaMwake. Kodi Iye akundiuza ine chiyani?”110 Ndipo ine ndinanyamula mfuti yanga, ndinapukutakanamulondolako, ndinayamba kuyenda chobwerera, kumapitachotsika phiri. Ndipo Chinachake chinanena kwa ine, “Bwanjiiwe osayenda ndi Ine kudutsamchipululu ichi, uyende ndi Ine?”

Page 29: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 29

111 Ine ndinati, “Inde, Ambuye, ndi mtima wanga wonse;ichi chikhoza kukhala chimodzi mwa zinthu zazikulukwambiri ine ndingachite, kuyenda ndi Inu.” Chotero inendinaika mfuti yanga pa phewa langa, ndipo ine ndinayambakuyenda kumatsika kudutsa pamenepo; panalibe nkhwangwainaikidwapo pamenepo, nkhalango yosakhudzidwa, ndikuyendakudutsa mmenemo.112 Ndipo pamene ine ndimatero, ndikuyenda mmenemo,kumatsika mtinjira ta zinyama ito, ine ndinamverera ngati, “inendikukhulupirira ine ndipita mpaka kumalo kumene…dzulolinali chikondwerero chathu, ndipo ine ndikaima pamenepobasi maminiti pang’ono; basi ngati sawasha pang’ono kwaMeda,pamene palimuluwamamba zogogoda, pamwamba pa chikwezachaching’onocho.” Ndipo ine ndinati, “Ine ndikukhulupirira inendiyenda kupita pamwamba pamenepo, basi ngati sawashaya chikondwerero chathu. Kenako ine ndibwerera kumbaliina iyi, mu nkhalango zowirira izi, ndi kuyenda mozungulira,ndi kupita mozungulirabe, kulowera ku Nsonga za Corral, ndikudzabwereranso kutsika njira imeneyo.” Basi kumangoyendandi kusangalala.113 Ine ndimati, “Atate, ine ndikudziwa Inu mukuyenda ndi ine.Ndipo ndi chamwayi bwanji; palibe wamkulu aliyense yemweine ndingamayende naye; Mulungu weniweniyo!” Ndi kuwalakwa dzuwa lofunda kuja!114 Ngakhale pamene ine ndinadzatsika mapiriwo. Inendinadzaima pomwetsera mafuta, ndipo ine ndinati, “Tsikulokongola!” Patadutsa masiku atatu. Siinagwe mvula deralimenelo la dziko kufikira masiku anaiwo atatha. Dzuwalimawala tsiku ndi tsiku. Nkulondola uko, abale? [Abaleakuti, “Ameni.”—Mkonzi.] Mukuona? Ndipo opanda mtambommwamba.115 Ndipo ine ndinafika pomwetsera mafuta, ine ndinati,“Ndithudi tsiku lokongola.”

“Inde, ilo liri!”Ine ndinati, “Kwakhala kuli kowuma kwambiri.”

116 Anati, “Ndi chinthu chachilendo!” Womwetsera mafuta uyuanati, anati, “Inu mukudziwa, iwo anatiuza ife kuti tikhala ndinkunthowaukulu, komamwadzidzidzi iwo unadzasiya!”117 Ine ndinatsikira, mpaka ku mzere wa New Mexico. Billy ndiine, mwana wanga, ife tinapita ku malo aang’ono kumenekokuti tikapeze zina…mmawa umene ife tinanyamuka, ndipo inendinati, “Ndithudi tsiku lokongola.”

“Inde, ilo liri!”Ine ndinati, “Kukuwoneka ngati kwakhala kuli kowuma

kwambiri.”“Inde, kwakhaladi choncho!”

Page 30: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

30 MAWU OLANKHULIDWA

Ine ndinati, “Kodi ndinu ochokera kuno?”118 Anati, “Ayi, ndine wochokera ku Wisconsin,” kapenakwinakwake. Anati, “Ine ndakhala ndiri kuno pafupifupi zakatwente, chotero ine ndikuganiza iwe ukhoza kukutcha ikokwanu.”119 Ine ndinati, “Ndinu mzika ndiye, ine ndikuganiza.” Choteroine ndinati, “Inde, bwana,” ine ndinati, “zikuwoneka ngatikwakhala kuli kwafumbi kwambiri.”120 Anati, “Inu mukudziwa, chinthu chodabwitsa kwambirichachitika!” Anati, “Ife tinali ndi kulengeza kwa zanyengokuti tikhala ndi nkuntho, chisanu chambiri; ndipo ndithudizinayambika, ndipo kenako nkudzasiya!”121 Ine ndinati, “Inu musamanene choncho,” ndipo mofatsilirakwambiri.122 Ndipo ine nditabwera kunyumba. Ndipo M’bale Tomananena kuti iye anauzidwa kuti asadzere njira imeneyo,nkuntho unali utatha. Ndipo iye anabwera kudzera komweko,kunalibe ngakhale dontho la mvula kapena chirichonse! Iyeadakali Mulungu, mwaona, basi monga mmene Iye nthawizonsewakhala akukhalira. Mukuona?123 Ndikuyenda kumeneko, ine ndimapita kumeneko…Tsopano, gawo ili, ine ndikuyembekeza mkazi wanga saipezatepi iyi. Mukuona? Koma ine ndikuuzani inu chinachake. Ndipo,tsopano, ine—ine sindikuuzani inu…Ine ndimangokuuzaniinu Choonadi, mwaona, ndipo ndiyo njira yokhayo yochitiraizo. Ine kawirikawiri ndimadabwa chifukwa chiyani iyesadandaula kuti ine ndimapita maulendo amenewo pachikondwerero chathu. Inu mukudziwa zimene ine ndimaganizammalingaliro anga? Ine ndinati, “Kumakhala anthu ambirikunyumbako. Ndiyeno ine nthawizonse, inu mukudziwammene ine ndimakhalira, wamanjenje. Ndipo zonse zimene inendimayankhula, ine ndimafuna kuti ndiziyankhula, zaMulungu,Baibulo, kapena chinachake. Mwinamwake iye amaganiza kutikumakhala kupuma pang’ono kwa iyeyo. Iye amandisiya inemasiku pang’ono, kuti ndipite kokasaka.” Ine, ndimakhalandikuganiza pang’ono zimenezo, ndikupita kumeneko.124 Izo, ndine…ine, ine ndikampepesa iye, ndipo ndine—inendamupempha Mulungu kuti andikhululukire ine chifukwa chakuganiza koteroko. Chifukwa, ine ndikuyenda kumeneko, inendinaganiza, “Chabwino, iye akuganiza…Chabwino, kalangaine! Iye, iye amagwira ntchito, inu mukudziwa, ndipo—ndiponthawizonse pamene iye ali ku khitchini kapena kwinakwakepanja uko…”125 Ndipo aliyense wa inu mumamudziwa iye, makina ochapirazovala amenewo amakhala akugwira ntchito nthawizonse.Ndipo kotero ine ndimapita, ine ndimakamukoka iye; ine nkuti,“Usamachape monga choncho. Tandiyankhula ine. Ukuwona,

Page 31: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 31

ine ndimakukonda iwe. Ine ndikufuna kuti iwe undiuze inechinachake; undiuze ine iwe umatero, nawenso.”126 Iye anati, “Chabwino, iwe ukudziwa ine ndimatero,” akateronkumapitirira kuchapa mwamphamvu mmene iye nthawizonseamachitira.127 “Ine sindifuna kuti iwe uzichita zimenezo. Ine ndimafunakuti iwe uzibwera kuno ndi kudzakhala pansi pafupi ndi ine.”128 “Oh, Bill, ine ndiri ndi ntchito yambiri yoti ndichite!”129 Ndipo ine ndinaganiza, “Chabwino, ndawona, ndikamapitauko, iye amapeza nthawi yoti azigwira ntchito zake.” Ndikupitauko, ndikuganiza zimenezo.

Tsopano, kumbukirani, ine ndaika Baibulo ili apa kuti inumuwone kuti ine ndaima patsogolo paMawu.

Pamene ine ndinali kuyenda pamenepo, chinachakechinandichitikira ine. Ine ndinayamba…130 Choyamba, ine ndinali kuganiza za pamene inendinamutengera iye kokakhala kwatokha kumeneko. Iye analimtsikana wokongola, wamng’ono, wa tsitsi lakuda, wa masoa bulawuni, ndipo ine ndinkamunyamula iye pomudutsitsa pazipika izi, inu mukudziwa, ndi chirichonse, ndi kumayeserakumukweza iye kumeneko, malo awa kumene ine ndinalinditaphako chimbalangondo china. Ndipo ine ndinkafunandimusonyeze iye chimodzi, ndipo chotero…kumene inendinakapeza chimbalangondo ichi. Ndipo iye anali atavalansapato zanga zolishyira ng’ombe. Ndipo zimenezo ndipafupifupi zaka twente-thuu, kapena zaka twente-waniizo zisanachitike; zaka twente-thuu, ine ndikukhulupiriraizo zinali, zapitazo. Ife tinakwatirana mu 1941. Ndipo inendinkamunyamula iye, inumukudziwa, kudutsa pa zipika izi.131 Ndipo ine ndinaganiza, “Tsopano, kanthu kakang’onokosauka, kakupirirabe ndi ine, iye wachita imvi.” Eya. Inendinaganiza, “Chabwino,” ndipo ine ndinapita…[M’baleBranham akuyeretsa kummero kwake—Mkonzi.] Ndipoine ndinali ndisanamete kwa masiku pang’ono, ndipo inendinadzipeza kuti ndiri ndi imvi, nanenso! Ndipo ine ndinawonandevu zanga zikumabaya apa, za imvi, ndipo ine ndinaganiza,“Mnyamata wokalamba, iwe wangotsala pang’ono kuti uthetsopano. Mwaona, iwe, iwe uchita chirichonse, iwe kulibwinouchitemachawi. Iwe ukukalamba, nawenso.”Mukuona?132 Ndipo kotero pamene ine ndimapitirira monga chomwecho,chinachake chinachitika. Mwadzidzidzi, mu kusunthakulikonse, kachitidwe, ine ndinali mnyamata, ine ndimaganizangati mnyamata. Ndipo ine ndinali nditaweramitsa mutu wangapansi, ndipo ine ndinayang’ana mmwamba. Ndipo mowonekerabasi monga mmene ine ndimamuwonera iye, iye anali ataimapamenepo atatambasula manja ake. Ndipo ine ndinaima;

Page 32: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

32 MAWU OLANKHULIDWA

ndinapukuta kumaso kwanga. Ine ndinayang’ana. Ine ndinati,“Meda, kodi ndi iweyo, Wokondedwa?”133 Ine ndinayang’ana apa, ine ndinaganiza, “Tsopanochachitika ndi chiyani?” Ndipo ine ndinaganiza, “Inde,ine ndikuyenda ndi Iye.” Ndipo izo zinasintha pamenepo,ine ndinabwereranso kukakhala bambo wokalamba, ndipomasomphenyawo anandichokera ine.134 Ndipo ine ndinaima; ine ndinavula chipewa changakachiwiri, ndinachiika icho pa mtima panga. Ine ndinati, “Yesu,mtima wanga wakhala wolemedwa kwambiri, kwa zaka. Inesindikusowa kuti ndikuuzeni inu kuti ine ndalemedwa. Inendalapa, ine ndalapa, ine ndachita chirichonse chimene inendikuchidziwa. Ndipo ndi chifukwa chiyani kulemedwa ukusikukundichokera ine?”135 Ndipo ine ndinangoyamba kumapitirira kuyenda. Ndipopamene ine ndimakwera nsonga yaing’ono iyi, pafupifupimayadi sate, forte kutsogolo kwanga; ine ndinayamba kukweransonga iyi, ine ndinayamba kudzimva kufooka kwenikweni.Ndipo apo panali mamba yogogoda yaing’ono, ya pafupifupimainchesi teni ikudutsa, inadzakwera ndipo inadzapangaL, ndipo kenako inadzakweranso. Ndipo basi pamene inendinakafika pamenepo, ine ndinadzimva kufooka kwambiri inendimadzandima. Chotero ine basi…ine ndinali nditavalansochipewa changa. Ndipo ine ndinangotsamiritsa mutu wangapa uwu; unangondikwana ine bwino bwino, kuyika mutuwanga pomwe apa pa mamba yaing’ono yogogoda ija, mongachonchi. Iyo ndi yolibwidika ndithudi. Iyo ili ngati, imawonekangati chitimbe, inu mwaona. Ndipo ndi…ine ndinatsamirapamenepo. Ndipo ine ndinangoima pamenepo ndi mutuwanga nditaweramitsa pansi, dzuwa lotentha mofunda ilolikundiwotcha ine pa nsana. Ndipo ine ndikuganiza, “Mulunguyemwe uja, amene anasamutsamvula ndimphepo ija!”136 Ndipo ine ndinamva chinachake chikuyenda, “pha, pha,sipha.”137 Ine ndinaganiza, “Ndi chiyani chimenecho? Madzi onseapita. Dzuwa latuluka. Kodi sipha ameneyo ndi chiyani?”Ine ndinayang’ana pansi; anali madzi ochokera m’masomwanga momwe, akudutsa kutsikira mndevu zanga za imvindi kumagwera pa masamba owuma amene Mulungu analiatawaumitsa, ali patsogolo panga. Ine ndinangoima pamenepomonga chonchi, basi nditatsamira mtengowo. Dzanja langa,dzanja ili pansi, mutu wanga nditatsamiritsa mtengo, dzanjalanga pa chingwe cha mfuti, monga chonchi, nditaimapamenepo, ndikulira.138 Ine ndinati, “Mulungu, sindine woyenera kukhala wantchitoWanu.” Ndipo ine ndinati, “Ine, ndikupepesa, ine—ine ndapangaa…Ine ndapanga zolakwitsa zambiri. Ine sindimatanthauza

Page 33: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 33

kuti ndizilakwitsa, Ambuye. Inu mwakhala wabwino kwambirikwa ine.”139 Maso anga nditatseka; ndipo ine ndinamva chinachakechikuyenda, “stompu, stompu; stompu, stompu.”140 Ine ndinakweza maso anga, ndipo nditaima patsogolopanga pomwe panadzabwera agwape atatu. Ndipo inendinaganiza, “Apo pali ya M’bale Evans imodzi, ya M’baleWood. Ndipo apo pali agwape atatu, mwaona, basi amene inendimawafuna.” Tsopano, mvula yauma; ine ndinafikira kutindikatenge mfuti yanga. Ine ndinati, “Ine sindingachite izo. Inendinamulonjeza Mulungu kuti ine sindimachita izo.” Mukuona?“Ine ndinamulonjeza Iye sindimachita izo.”141 Ndipo chinachake chinanena kwa ine, “Koma ndi awo aliapowo!”142 Ndipo ine ndinaganiza, “Inde, Sa-…Ndi chimene a—munthu anamuuza Davide, nthawi ina, ‘Mulungu wamuperekaiye, ine ndinati, mmanja mwako!’” Inu mukudziwa, MfumuSauli.143 Ndipo Yoabu anamuuza iye, anati, “Umuphe iye! Iyewagona apo!”144 Ndipo iye anati, “Mulungu asalole kuti ine ndikhudzewodzodzedwa Wake.”145 Ndipo agwape amenewo anaima pamenepo ndipoamandiyang’ana ine. Ndipo ine ndinaganiza, “Iwo sangathawe.Palibe njira yoti iwo angathawire. Iwo siali mayadi satekutalikirana ndi ine. Ndipo ine ndiri ndi mfuti iyi, ili apayi,ndipo apo pali agwape atatu. Ayi, ine sindingachite zimenezo.Ine—ine basi sindingachite zimenezo.” Iyo inali manthu nditiana tiwiri. Chotero ine—ine—ine sindimatha basi kuti nditengemfuti. Ine ndinati, “Ine sindingathe.” Ine—ine sindinasunthenkomwe. Ine ndinangokhala pamenepo. Ine ndinati, “Inesindingachite zimenezo, chifukwa ine ndinamulonjeza Mulunguine sindidzachita izo. Ngakhale, abale amenewo, iwo—iwosakusowa agwape awo. Mukuona? Ine—ine sindingachite ichi.Ine basi sindingachite ichi.”146 Ndipo manthu ameneyo anabwera, anayenda. Tsopanomvetserani, kunali kuli amuna zana akuwombera pa iwokumeneko, kwa masiku anai kapena asanu. Zowopsya?Chizindikiro choyamba cha chofiira…Ndipo ine ndinalinditavala malaya ofiira, chipewa chofiira. Chizindikirochoyamba, izo zithawa; koma izo zinali zitaima pamenepo, zonsezitatu za izo, zikuyang’ana pa ine.147 Ine ndinati, “Mayi, tenga ana akowo ndipo kazipitamu tchiremo. Iwe uli mmanja mwanga. Ine…Moyo wakouli mmanja mwanga, koma ine sindikuvulaza iwe. Inendinamulonjeza Mulungu kuti ine sindimatero.” Mukuona?

Page 34: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

34 MAWU OLANKHULIDWA

Ndipo iye anayenda moyandikira. Iye amatha kundiyang’anaine. Zonsezo zinayenda mondiyandikira, mpaka izozinayandikira kwambiri mwakuti izo zikanakhoza kudzadyerammanja mwanga, pafupifupi. Izo, ndipo mphepo ikuwomba paizo. Chotero iyo inapotoloka, inabwerera m’mbuyo pang’onoiliyonseyo, zitatu zonsezo.148 Ndipo apo iyo ikubwereranso, kuyenda kubwera kwa ine.Ine sindinasunthe nkomwe; ndinangoima pamenepo. Ine ndinati,“Kazipitani mu tchire; ine ndimakondamonso, chimodzimodzi.Kakhaleni moyo! Mwaona, moyo wanu uli mmanja mwanga,koma ine ndakusiyani inu. Inu simukanatha kuthawa. Inumukudziwa inu simukanatha.” Ine ndikhoza kupha zitatuzonsezo basi mu mphindi imodzi, mphindi zitatu, mulimonse,mwaliwiro basi mmene ine ndingathe kuwombera; ndipo izosizikanatha kuthawa, zitaima pafupi ndi ine. Mukuona? Ndipoine ndinati, “Ine ndakusiyani inu. Pitani, mukakhale moyo.”Ndipo ine ndinaima pamenepo. Izo zinapita zikuyenda, zinapitampaka mtchire.149 Ine ndinapukuta nkhope yanga monga choncho,ndipo basi pomwepo chinachake chinachitika. Liwulinayankhula, momveka bwino basi, kuchokera mumlengalengamwabuluu umo, mopanda mtambo. Izo zonse zinali mkatimwa pafupifupi…basi kanthawi pang’ono. Ndipo Liwulinayankhula momveka, ndipo linati, “Iwe unakumbukiralonjezo lako, sichoncho iwe?”150 Ine ndinati, “Inde, Ambuye.”151 Iye anati, “Ine ndikumbukira Langa, inenso. ‘Inesindidzakusiya iwe kapena kukutaya iwe.’” Kulemedwakokunachoka pa mtima wanga. Iko kwakhala palibepo kuyambirapamenepo; iko kusadzabwererenso kachiwiri.152 Kenako ine ndinabwera kuTucson. Chinthu chachilendo, inesindinakhalepo ndi zochitika zochuluka kwambiri, kuyambirapamene ine ndinabwera kuno. Ine—ine ndikukhulupirira analiMulungu akundigwirira ora limenelo. Ine ndikukhulupirira kutinthawi tsopano ili pafupi, kuti chinachake chichitike.153 Ngati ife titangokhoza kulandira Choonadi ichi! Tsopanokwa mphindi chabe. Ngati ife tikanangozindikira chimeneLemba ili likutanthauza, “Iye amene ali mwa inu ndi wamkulukuposa iye amene ali mdziko.” Ife timalephera kuti timvetseIchi, komabe ife timanena kuti ife timakhulupirira Ichi.Ndipo ife tikudziwa kuti Icho ndi choona, koma ife ndithudisitimachimvetsa Icho.

…wamkulu ali iye amene ali mwa inu, kuposa iyeamene ali mdziko.Nchiyani chimene chiri mwa inu, chimene chiri chachikulu?

Ndi Khristu, Wodzodzedwayo! Mulungu, amene anali mwa

Page 35: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 35

Khristu, ali mwa inu. “Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu,kuposa iye amene ali mdziko.”154 Ndiye ngati Iye ali mwa inu, si inunso aponso amenemukukhala moyo, ndi Iyeyo akukhala moyo mwa inu. Mukuona?Si kuganiza kwanu, chimene inu mungaganize chokhudza Ichi;ndi chimene Iye ananena za Ichi. Mukuona? Ndiye, ngati Iye alimwa inu, Iye mwamtheradi sangakane chimene Iye ananena. Iyesangachite izo. Koma Iye angasunge chimene Iye wanena, ndipoIye akuyesetsa kuti amupeze munthu ameneyo amene Iye athakuzitsimikiziramo Yekha.155 Tsopano, zimenezo sizikutanthauza kuti Iye akuyenera kutiachite izo kwa aliyense. Mu nthawi imene Mose anatsogoleraana a Israeli, kunali mmodzi, ameneyo anali Mose. Enaonsewo ankangotsatiraUthenga.Mukuona? Ena a iwo anayeserakuti adzukepo kuti akakopere izo, ndipo Mulungu anati,“Dzilekanitse wekha,” ndipo anangowamezapo iwo. Mukuona?Mukuona?156 Tsopano, koma, “Iye amene alimwa inu ndiwamkulu kuposaiye amene ali mdziko,” Mulungu mwa inu, chimodzimodzimonga Iye anali mwa Yesu Khristu. Chifukwa, zonse zimeneMulungu anali, Iye anadzitsanulira mwa Khristu; ndipo zonsezimene Khristu anali, Iye anadzitsanulira mu Mpingo. Mwaona,ameneyo ndiMulungumwa inu, “Iye amene ali mwa inu.”157 Nzosadabwitsa mphepo ndi mafunde zinamumvera Iye,zinamvera Mawu Ake; zinamvera Mawu Ake, chifukwa Iwoanali Mawu a Mulungu kudzera mwa Iye. Iye anali Munthu;koma Iye anali Mawu, osandulika thupi. Mukuona? Ndipopamene Iye ayankhula, amakhala Mulungu akuyankhulakudzera mmilomo ya munthu. Mukuona? Nzosadabwitsamphepo ndi mafunde…Mlengi weniweniyo, amene analengamphepo ndi mafunde, anali mwa Iye. Tsopano, taganizani zaizo! Muganize mwakuya tsopano, ndisanafike ku mphindi iyiyotsekera. Nzosadabwitsa ziwanda zimapuwala pa Mawu Ake!Anali Mulungu mwa Iye. Anali Mulungu mwa Khristu. Ziwandazimapuwala. Nzosadabwitsa akufa, amene amabwerera kufumbi, samatha kukhala pamenepo, pa Mawu Ake! Pakuti,Iye anali Mawu.

Iye ananena kwa Lazaro, atamwalira ndipo akununkha,masiku anai; nkhope yake, mphuno, zinali zitagwera mkati,mu nthawi yochuluka chomwecho. “Lazaro, tuluka!” Ndipomunthu, wakufa, anadzuka pa mapazi ake. Chifukwa chiyani?Anali Mulungu. Iye amene anali mwa Khristu anali Mulungu.Akufa samatha kuima mu Kukhalapo Kwake. Anali Mulungumwa Khristu.158 Mphepo, tsopano, kumbukirani, Mulungu analenga mphepo;ndi mpweya. Mulungu analenga mafunde; ndi madzi. Komapamene mdierekezi anadzalowa mmenemo, iye anawavundula

Page 36: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

36 MAWU OLANKHULIDWA

iwo, kuti abweretse chiwonongeko. Mulungu analenga anthu,kuti adzakhale ana aamuna a Mulungu, koma pamenemdierekezi alowa mwa iwo, mwaona, pamakhala vuto. Tsopano,ameneyo anali mdierekezi amene anadzalowa mu mphepozozimene zinatumiza nkuntho uja. Kodi Mlengi, amene analengamphepo, sakanati, “Bwerera kumene ine ndinakulengera iwe”?

Kodi uyo si Mlengi yemwe uja amene anali ataimirirapa phiri la Colorado tsiku lina? [Osonkhana akuti,“Ameni.”—Mkonzi.] Mukuona?

Kodi uyo si Mmodzi yemwe uja amene amatha kutengachidutswa cha nsomba ndi kuinyema iyo, ndipo chidutswa chinankumerapo? Iye kwenikweni sankasowa kuti achite kukhalanayo iyo. Iye akanatha kungonena izo.

Kodi ameneyo si Mlengi yemweyo amene analengaagologolo? [Osonkhana akuti, “Ameni.”—Mkonzi.] Ndiye, Iyeamene anali mwa Khristu ali mwa ife, mwaona, pakuti Iyeakuchita ntchito zomwezo zimene Iye ankachita, chinthuchomwe chomwecho.

Akufa samatha kuimamuKukhalapoKwake, paMawuAke.159 Taonani, ife tiri ndi maneno asanu otsimikizika, a anthu“akufa,” ndipo Ambuye nkupereka masomphenya, ndiponkupita kwa iwo ndi kukawadzutsanso iwo. Apa pakhalawina, pomwepano tsopano, amene anafa pomwepo pamene iyewakhala apo. Ndipo pano ndi uyu ali moyoyu, usikuuno; anagwandi nthenda ya mtima. Apo pali mkazi wake, namwino. Ifetinapita uko; chirichonse chinali chitapita, maso ake anakhala,ndipo anapita. Ndi uyu ali apayu, wamoyo. “Pakuti wamkuluali Iye amene ali muno, mwa ife, kuposa iye amene ali mdziko!”Mukuona?160 Wamkulu ali Iye! Ndi Mulungu, Mlengi! Mphepondi mafunde zimayenera kuti zimumvere Iye. Ziwandazimapuwalitsidwa. Chirengedwe chonse chimamumvera Iye,chifukwa Iye anali Mlengi wa chirengedwe. Oh, pamene ifetiganiza zimenezo, izo zimachotsapo ukali. Ndiye ife timamvetsazinthu izi, inumwaona. Ndi chiyani icho? Simunthu ayi.Munthusangathe kuchita zimenezo; munthu ndi gawo la chirengedwe.Mukuona?Komandimphepo ndimafunde zimene zimamumveraMlengi. Mukuona?

Ndipo zimatengera Mlengi kuti achite zimenezo, “PakutiIye amene ali mwa inu ndi wamkulu kuposa iye amene alimdziko.” Iye amene akhoza kuyambitsa chisokonezo, ameneyondi iye amene ali mdziko. Iye amene ali mwa inu, ndi Mlengi,Amene anapanga mphepo. Iye atha kumudzudzula mdierekezikuti atuluke mu mphepo, ndipo apo nkukhala bata. Iye akhozakumudzudzula mdierekezi atuluke mu nkuntho, ndipo apoosakhalapo nkuntho. Iye ndi Mlengi. “Ndipo wamkulu ali Iyeamene alimwa inu, kuposa iye amene alimdziko.”Mukuona?

Page 37: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 37

161 Mdierekezi ndi wa dziko lapansi. Dziko linali la iyeyo.Ilo nthawizonse lakhala liri lake. “Chifukwa chiyani iwewagwa, O Lusifara, mwana wa mmawa?” Mwaona, dziko ili ndilake. Pamenepo ndi pamene iye, anathamingitsidwa kuchokeraKumwamba, iye anabwerera kwa ilo. Mukuona?162 Anali iyeyo yemwe ananena kwa Khristu, “Maufumu awandi anga, ine ndimachita nawo iwo monga ine ndifunira.” Iwondi a iyeyo, ndipo ndi iyeyo yemwe “ali mdziko lapansi.”163 Yohane anali atangowauza ophunzira, “Inu munamva zawotsutsakhristu amene alinkudza, ndipo iye ali kale kunoakugwira ntchito mwa ana a kusamvera. Koma, ana aang’ono,inu simuli a dziko lino. Ndinu a Mulungu. Ndipo wamkulu aliIye amene ali mwa inu, kuposa Iye amene ali mdziko.” Ameneyondi Khristu mwa inu!164 Iye amene—amene analenga miyamba ndi dziko lapansi,anadzawonetseredwa mwa Munthu wa Yesu Khristu; MulungumwaKhristu, akuyanjanitsa dziko kwa Iyemwini.

Tiyeni tinene kuti inu mukuti, “Ameneyo anali Mwana waMulungu, naponso, M’bale Branham.” Chabwino, tiyeni tipezengati Iye ali Wamuyaya, Mulungu wosatha.165 Wamkulu anali Iye amene anali mwa Yoswa, kuposadzuwalo. Ndipo Yoswa anali munthu, wobadwa mu tchimo,monga inu ndi ine. Ndipo wamkulu anali Iye amene analimwa Yoswa, ndi mu dzuwa limene linkayendera lamulo laMulungu. Mulungu analilamulira dzuwa limenelo kuti liwalendipo linadzitembenuza lokha, ndipo limayendetsedwa ndikulamuliridwa ndi malamulo a Mulungu. Koma wamkulu analiIye amene anali mwa Yoswa, kuposa chimene malamulo aMulungu anali; chifukwa Mlengi, Mwiniwake, amakhala mwaYoswa pamene Yoswa anayang’ana mmwamba kwa dzuwandipo anati, “Iwe uime pamene iwe ulipo. Ndipo, mwezi, iweupachikike pamenepo pamene iwe ulipo, kufikira ine ndimalizenkhondo iyi.” Ndipo dzuwa ndi mwezi zinamumvera iye, pakutiIye amene anali mwa Yoswa anali wamkulu kuposa dzu—dzuwandi mwezi. Iye amene anali mwa Yoswa!166 Iye amene anali mwa Mose, anali wamkulu kuposa Igupto.Igupto anali magulu ankhondo amphamvu a mdziko, iwo analiatagonjetsa dziko lapansi pa nthawi imeneyo. Koma wamkuluanali Iye amene anali mwa Mose, kuposa Igupto inali, chifukwaMose anagonjetsa Igupto. Wamkulu anali Iye amene analimwa Mose, kuposa ngakhale chirengedwe icho chomwe. Kodiinu munayamba mwaganizapo kuti Mulungu anatenga MawuAke ndipo anawapereka Iwo kwa Mose, ndipo anati, “Pitauko ndipo ukalamulire kuti dzuwa lisawale”? Ndipo dzuwalinachita mdima! Nkulondola uko? Iye akhoza kupangitsadzuwa kuwala ndi mitambo kubwerera, kapena Iye akhozakulipangitsa dzuwa kukhala lakuda. Iyeyo ndi Mulungu; Iye

Page 38: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

38 MAWU OLANKHULIDWA

akhoza kuchita chirichonse chimene Iye akukhumba, ndipo Iyeakukhalamwamwanawokhulupirira! Ameni. Ndi zimenezotu.167 Panalibe utitiri powonekera. Zikhoza kukhala kuti inalinthawi yachisanu, kunalibeko ntchentche, koma Mulunguanati kwa Mose, “Pita ukayankhule Mawu Anga, ndipo Inendikaika mmalingaliro ako choti ukanene. Ndipo iwe upitekumeneko ndipo ukatenge dothi lina kuchokera mnthaka, ndipoukaliponyere ilo mumlengalenga, fumbi.”168 Ndipo anati, “Pakhale utitiri!” Ndipo utitiri unaliukukwawa mwina pafupifupi mainchesi angapo kuya kwake,ponseponse pa nthakapo, mu maora pang’ono. Nkulondola uko?Mlengi!169 Kunali kulibe achule aliwonse, chotero iye anatambasulandodo yake ndipo anati, “Pakhale achule!” Ndipo iwoanali ponseponse, anawunjikana, kufikira dziko lonse linalikununkha. Nkulondola uko?170 Pamene anafika pa Nyanja Yofiira ndipo iyo inali mu njirayake, Mulungu anati, “Yankhula kwa nyanja.” Ndipo Moseanayankhula kwa nyanja; ndipo Wamkulu ali Iye amene analimwa Mose, kuposa chimene nyanja inali payokha. Nkulondolauko? Oh, mai! Tsopano, inu mwaona, wamkulu anali Iye ameneanali mwa Mose, kuposa iye amene ali mdziko. Wamkulu aliIye amene anali mwa Mose, kuposa chirengedwe chirichonsechimene chiripo mdziko. Iye analamulira chirengedwe. Pachirichonse chimene Mulungu anamuuza iye kuti anene, iyeanachinena icho, ndipo ndi mmene izo zimachitikira.171 Mulungu yemweyo ali ndi ife usikuuno! Osati kokha ndiife, koma mwa ife! Iye watsimikizira kuti Iye anali mwa ife.“Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu, kuposa iye amene alimdziko.” Kodi ife tikuwopa chiyani, dziko lapansi?172 Kuno tsiku lina iwo anapeza a—a mtundu wina wa dzinola dinosara, chakuno pafupi ndi…Ine ndikuganiza inu nonsemunamva za izo; chakuno ku Mathithi a Niagara. Anati, “Ilolimalemera mapaundi sikisi.” Ine ndimaganiza kuti iwo anenakuti ilo lachokera kwa munthu, koma ine—ine ndikuganizaiwo potsiriza anachifotokoza icho kuti ndi chinyama chinacha makedzana. Zinyama zimenezo mwinamwake zinakhalaponthawi ina pa dziko lapansi. Kodi izo ziri kuti tsopano?

Kodi inu mukudziwa, Mulungu Wamphamvuzonse akhozakulamulira madinosara kuti abwere pa dziko lapansi lino,mu ora likubwerali iwo nkudzakhala mamailosi forte kuyakwake? Inu mukudziwa, Mulungu akhoza kuliwononga dzikolino ndi utitiri? Iye akhoza kuitana utitiri. Kodi iwo umapitakuti ukafa? Kodi chimachitika ndi chiyani kwa ntchentche?Kodi chimachitika ndi chiyani kwa chiwala? Nyengo yachisanuikabwera, ndipo kumakhala forte pansi pa ziro; ndipo, mukapitamchirimwe chotsatira, ziwala ponseponse. Kodi izo zimachokera

Page 39: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 39

kuti? Iye ndi Mlengi amene amayankhula izo kuti zikhalepo! IyendiMulungu! Chirengedwe chimamveraMawuAke.173 Pamene abale athu ambiri amatengeka, iwo amakhutitsidwakuti Mulunguwanena kuti achite chinthu chinachake, ndipo iwoamati ndi PAKUTI ATERO AMBUYE pamene izo si ndizo. Ichonchifukwa chake izo sizimachitika.

Koma pamene zikhala kuti ndi Mulungu ndithudiakukuuzani inu, izo zimayenera kuti zichitike, izo zimayenerakuti zikhale mwanjira imeneyo. Mukuona? Pamene Mulunguayankhula izo, izo zimayenera kuchitika.174 Wamkulu ali Iye amene anali mwa Mose, kuposa Iye ameneanali mu Igupto. Wamkulu ali Iye amene anali mwa Mose,kuposa chirichonse chimene Farao akanachita, matsenga akeonse. Wamkulu anali Iye amene anali mwa Mose, kuposa iyeamene anali mwa amatsenga. Mukuona? Wamkulu anali Iyeamene anali mwaMose, kuposa chirengedwe chonse.175 Wamkulu! Iye amene anali mwa Danieli anali wamkulukuposa mikango. Iye anatha kuiyimitsa mikango yanjalaija. Chotero chirichonse chimene chingaimitse chirichonse,chimakhala chachikulu kuposa chimene iye anachiyimitsacho.Chotero mikango anaikhwiyitsira, yanjala, kuti imudye Danieli;ndipo wamkulu anali Iye amene anali mwa Danieli, kuposa iyeamene anali mwa mkango.176 Tsopano, pamene mkango unalengedwa poyambirira, iwounali bwenzi wa munthu. Ndi mdierekezi amene amampangitsaiye kuchita zimenezo. Uko nkulondola. Mu Zakachikwi,nkhandwe ndi mwanawankhosa zizidzadyera pamodzi,ndipo mkango uzidzadya udzu ngati mwana wang’ombe,ndipo uzidzagona limodzi ndi mwana wang’ombe. Izosizidzamapwetekana kapena kuwonongana mu Zakachikwi.Mdierekezi adzakhala atapita. Ndi mdierekezi yemweamapangitsa zinyama zakuthengo kung’ambana ndikukhadzulana ndi kudyana, ndi zinthu monga choncho, mmeneizo zimachitira. Ndi Satana amene amachita zimenezo. Komawamkulu anali Iye amene anali mwa Danieli, kuposa iye ameneanali mwa mkango. Mukuona? Wamkulu anali Iye amene analimwamneneri, kuposa iye amene anali mwamkango.177 Wamkulu anali Iye amene anali mwa ana a Chihebri,wamkulu anali Iye amene anali mwa iwo, kuposa iye ameneanali mu moto. Pakuti iwo anaponyedwa mmoto; ndipo Iyeamene anali mwa iwo, anali ndi iwo, ndipo analepheretsamoto kuti usawawotche iwo pamene ng’anjo inatenthetsedwakasanu ndi kawiri kutentha kuposera mmene iyo imatenthera’,kutenthetsedwa. Kulondola uko?Wamkulu anali Iye amene analindi ana a Chihebri, kuposa iye amene anali mdziko.178 Apo panakhala Nebukadinezara, kapena Belitsazara.Nebukadinezara, ine ndikukhulupirira anali iyeyo, amene

Page 40: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

40 MAWU OLANKHULIDWA

anatenthetsa ng’anjo kasanu ndi kawiri kuposera mmeneimakhalira. Anadzodzedwa ndi mdierekezi, kuti awatengeanthu awa, chifukwa iwo amaima ndi Mawu a Mulungu; ndipoanawaponyera iwo mu ng’anjo iyi, kasanu ndi kawiri kutenthakuposera mmene iyo imakhalira konse, ndipo iyo siinawatenthenkomwe iwo. Pakuti wamkulu anali Iye amene anali mwaShadreki, Misheki, ndi Abedinego, kuposa iye amene ali mdziko.Mwamtheradi! Oh, mai!

179 Wamkulu anali Iye amene anali mwa Eliya, kuposamumlengalenga mwa mkuwa, chifukwa iye anatha kubweretsamvula kuchokera mu mlengalenga mwa mkuwa imene inaliisanavumbe kwa zaka zitatu ndi miyezi sikisi.

Wamkulu ndi Iye amene anali mwa Eliya, kuposa imfa.Pakuti, pamene inafika nthawi yakuti iye afe, Mulunguanamuwona mneneri wakale, wotopa uja. Iye anakhalaakumudzudzula Yezebeli ndi mapenti ake onse ndi zinthuzamakono, ndipo iye anali ngati atatopa, chotero Iye sanamulolenkomwe kuti iye azipita kwawo,monga Iye anachitira ndi Enoki.Iye anatumiza galeta ndipo anamutengera iye mmwamba, ndikumutengera iye Kwawo. Wamkulu ali Iye amene anali mwaEliya, kuposa iye amene anali mu Yerusalemu ndi mu Yudea,ndi mmapiri. Wamkulu anali Iye amene anali mwa Eliya, kuposaimfa payokha. Wamkulu anali Iye amene anali mwa Eliya,kuposa manda; chifukwa iye anazemba manda, iye anaizembaimfa, ndipo iye anangopita Kwawo pa galeta. Mwaona, wamkuluanali Iye, ndipo Iye anali mwa Eliya.

180 Inu mukuti, “Oh, chabwino, ameneyo anali munthuwopambana.”

181 Dikirani miniti! Baibulo linati, “Iye anali munthuamene anali ndi zikhumbo,” chimodzimodzi mongainu ndi ine. Uko nkulondola. Koma pamene iyeamapemphera, iye amakhulupirira kuti walandira chimeneiye amachipemphereracho; chimene Yesu ananena kwa ife,“Pamene inu mupemphera, mukhulupirire kuti inu mulandirachimene inu mukuchipemphacho, icho chidzachitidwa.” Iyeanapemphera moona mtima kuti mvula isagwe, ndipo iyosiinagwe kwa zaka zitatu ndi miyezi sikisi. Mukuona? Wamkuluanali Iye amene anali mwaEliya, kuposa chirengedwe.

182 Ndiye nanga bwanji kuchiritsa wodwala? Mukuona?Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu, kuposa nthendayo.Mukuona? Chifukwa, uko nkusokoneza, kusokoneza malamuloomwe omwewo a Mulungu, nthendayo ili. Chabwino,“wamkulu” ali Iye amene ali mwa inu, ameneyo ndi Mchiritsindi Mlengi, kuposa a—kuposa mdierekezi amene wasokonezadongosolo kumene la moyo wanu. “Wamkulu ali Iye amene alimwa inu, kuposa iye amene ali mdziko.”Mukuona?

Page 41: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 41

Wamkulu anali Iye amene anali mwa Eliya! Wamkulu analiIye mwa Yesaya, kuposa nthawi inali; kapena aliyense waaneneri amenewo, chifukwa iwo amawona kudutsa nthawi.Mukuona?183 Wamkulu ali Iye amene anali mwa Yobu, kuposa ngakhalemphutsi za pakhungu, ndi imfa ndi manda. Chifukwa, mwamasomphenya iye anawona kubwera kwa Ambuye, ndipo anati,“Muomboli wanga ali moyo, ndipo pa tsiku lotsiriza Iye adzaimapa dziko lapansi; ndipo ngakhale mphutsi za pakhungu langaziwononga thupi ili, komabe mthupi langa ine ndidzamuwonaMulungu.” Mukuona? Wamkulu ali Iye amene anali mwa Yobu,kuposa imfa; wamkulu, chifukwa imfa inayesera kuti imutengeiye koma iyo siinakhoze kuchita izo. Iyo sikanakhoza kuchitaizo, chifukwa iye anati, “Ine ndidzaukanso kachiwiri,” ndipo iyeanatero. Iye anachita izo.184 Mvetserani, ndikukhumba ife tikanakhala ndi nthawi kutitipite patsogolo pa izi. Koma ine ndikufuna kufunsa funso,limene ine ndinamva likunenedwa tsiku linali, lokhudza,“Khristu mwa inu.”

Tsopano, musati—musalole izo zikhazikike pa chinachakechimene inu munachita; kuti, “Ine ndinamverera kunjenjemerapang’ono. I—i—ine ndinayankhula mmalirime. I—ine ndinavinamu mzimu.” Ndiribe chotsutsana ndi zimenezo, tsopano.Zimenezo ndi zabwino, mwaona, ndizo, koma musatimukhazikike pa zimenezo. Mukuona?

Moyo wanu ukuyenera kukhala Ichi. [M’bale Branhamakusasa Baibulo lake—Mkonzi.] Ichi ndi Chimenecho. Inu ndiIchi mukuyenera kusanduka chimodzi, mwaona, ndiyeno Ichichimadziwonetsera Chokha. Mukuona?185 Tsopano bwanji ngati—nanga bwanji ngati usikuunoinu mutati, ndi mtima wanu wonse, kuti mzimu waShakespeare ukukhala mwa inu, kuti Shakespeare akukhalamwa inu? Inu mukudziwa chimene inu mukanamachita? Inumukanamachita ntchito za Shakespeare. Inu mukanamakhoza.Inu mukanamakhoza. Inu mukanamapeka ndakatulo ndi—ndimasewero, ndi zina zotero, chifukwa Shakespeare anali walusowa mtundu umenewo, mlembi wamkulu, wolemba ndakatulo.Tsopano, ngati Shakespeare akanamakhala mwa inu, ntchito zaShakespeare inumukanamazichita. Nkulondola uko?186 Nanga bwanji ngati Beethoven akanamakhala mwainu? Bwanji ngati Beethoven akanamakhala mwa inu?Inu mukudziwa chimene inu mukanamachita? Inu bwenzimukulemba nyimbo ngati Beethoven, wopeka wamkulu. Inubwenzi mukanamalemba nyimbo ngati Beethoven, chifukwaBeethoven akanakhala moyo wanu. Inu mukanadzakhalaBeethoven, atabwereranso mthupi, kachiwiri. NgatiBeethoven akanamakhala mwa inu, ntchito za Beethoven inu

Page 42: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

42 MAWU OLANKHULIDWA

mukanamazichita, chifukwa Beethoven akukhala mwa inu.Nkulondola uko?187 Koma Iye amene ali mwa inu ndi Khristu! Ndipo ngatiKhristu ali mwa inu, ntchito za Khristu inu mudzazichita,ngati Khristu akukhala moyo mwa inu. Iye ananena choncho.Yohane Woyera 14:12, “Iye amene akhulupirira mwa Ine,ntchito zimene Ine ndikuzichita nayenso adzazichita,” ngatiinu munali mwa Khristu, kapena ngati Khristu akanamakhalamwa inu. Ndiye, Khristu ndi Mawu. Nkulondola uko? NdipoMawu amabwera kwa aneneri Ake. Mukuona? Ndipo ngati,inu, Khristu akanamakhala mwa inu, ntchito za Khristubwenzi zikuchitika kudzera mwa inu, Moyo wa Khristuukanamadzakhalidwa kudzera mwa inu. Ntchito zimene Iyeankazichita, moyo umene Iye ankaukhala, ndi chirichonse, izozikanamadzakhala moyo mwa inu; chimodzimodzi monga ngatiShakespeare, Beethoven, kapena—kapena aliyenseyo ameneakanamakhala moyo mwa inu.188 Ngati Moyo Wake! Koma ngati inu mukukhalabe moyowanu wanu, ndiye ntchito zanu zomwe inu mudzazichita.Mukuona? Koma ngati inu mukukhala Moyo wa Khristu, ngatiKhristu ali mwa inu, “Iye amene ali mwa inu ndi wamkulukuposa iye amene ali mdziko.” Ngati kukaikira kwanu ndizokhumudwitsa za lonjezo la Mulungu ziri mwa inu, ndiyeKhristu sali mmenemo; mwaona, inu mukungotengeka basi.Koma ngati Moyo, ngati Khristu akukhalamoyomwa inu, MawuAke Iye adzawazindikira ndipo lonjezo Lake Iye adzalichita.Mukuona? Iye adzachita.189 “Pamene inumupemphera, khulupirirani kuti inumulandirazimene inu mwapemphazo, ndipo izo zidzaperekedwa kwainu. Ngati inu mudzanena kwa phiri ili, ‘Suntha,’ ndipoosakaikira mumtima mwanu, koma kukhulupirira kuti chimeneinu mwanenacho chidzachitika, inu mukhoza kukhala nachochimene inu mwanena. Atate amagwira ntchito, ndipo inendimagwiranso ntchito momwemonso. Indetu, indetu, Inendinena ndi inu, Mwana sangachite kanthu mwa Iyeyekha;koma chimene Iye awawona Atate akuchita, chimenechoamachita Mwana momwemonso.” Mukuona? Ndipo pameneAtate anamuwonetsa Iye choti achite; anayenda kunja ukopopanda cholephera cha chirichonse, ndipo anati, “Kukhale,”ndipo zimachitika.

Ndipo Khristu yemwe uja akakhala mwa inu. Iye akakhalamwa ife. Ndiye ntchito Zake ife tidzachita, chifukwa Khristundi Mawu, ndipo lonjezo la Mawu limabweretsa machiritso kwainu. Kodi inu mukukhulupirira zimenezo? [Osonkhana akuti,“Ameni.”—Mkonzi.] Ndithudi!190 Iye anati, “Ine sindidzakusiyani inu ngati amasiye.” Pameneine ndipemphera, ndinafunsa kanthawi kapitako, kumeneko mu

Page 43: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 43

Mateyu 24, mwaona, kapena Mateyu 28:20. Mukuona? Iye anati,“Ine ndidzabwera kwa inu, ndidzakhala mwa inu. Ine,” Munthu,Khristu, mmawonekedwe a Mzimu Woyera, “ndidzabwera ndikudzakhala moyo mwa inu. Ndiye inu simudzakhala wanu—inu simudzakhala inu mwini aponso. Ine ndidzakhala mwa inu.Ndipo wamkulu ali Iye amene ali mwa inu, kuposa iye amene alimdziko.” Mukuona? Ahebri 13:8 amati, “Iye ali yemweyo, dzulondi kwanthawizonse.”191 Iye amene anali mwa Nowa anali wamkulu kuposa ziweruzoza madzi.

Ndipo Iye amene ali mwa inu ndi wamkulu kuposa ziweruzoza moto. Mukuona? Iye amene ali mwa inu ndi wamkulu,chifukwa Iye analipira chiweruzo ndipo anagonjetsa chiweruzommalo mwa inu. Mukuona? Palibe mantha za ichi. Mwaona, inumuli mmenemo. Inde.

Wamkulu ali Iye amene anali mwa Nowa, kuposa iyeamene anali mu ziweruzo za madzi, amene anawononga dzikolimene silinakhulupirire. Chifukwa, Nowa anakhulupirira.Ndipo wamkulu anali Iye mwa iye, amene anakhulupirira Iyeamene anayankhula ndi iye, kuposa iye amene anali mdziko.Mwakuti, Nowa anathawa chiweruzo chonse, chifukwa Mawua Mulungu anali aakulu kuposa icho, ndipo iye ananyamulidwapamwamba pa ziweruzo.

“Wamkulu!” Mmene ife tingakhale pa izo kwa kanthawi!Mukuona?192 Wamkulu ali Iye amene anali mwa Davide, kuposachimbalangondo chimene chinaba nkhosa yake.Wamkulu ali Iyeamene anali mwa Davide, kuposa mkango umene unabweramondi kudzatenga imodzi ya anaankhosa ake. Wamkulu ali Iyeamene anali mwa Davide, kuposa mdani, Goliati. Mfilisitiwamkuluyo amene anaima pamenepo, wamtalimapazi thwelofu,fortini, ndi zala mainchesi fortini pa iye; ali ndi nkondo ngaticholukira cha wowomba; ndipo ataphimbidwa paliponse ndichitsulo cha nchichi wa mainchesi awiri kapena atatu, chachitsulo kapena chiwaya, mkuwa. Koma chimene chinali mwaDavide chinali chachikulu kuposa chimene chinali mwa iye.

Iye anali mphamvu, minyewa. Iye anali wankhondo. Iyeamakhoza, monga anati iye akanamunyamula Davide ndinsonga ya nkondo wake ndi kumupachikapo iye, ndi kulolambalame kuti zimudye iye.193 Ndipo Davide anati, “Iwe ukukumana ndi ine ngati Mfilisiti,mu dzina la Mfilisiti. Iwe ukunditukwana ine mu dzina lamulungu wa Chifilisiti.” Ndipo anati, “Iwe wadzibwekererachimene iwe uti uchite. Ndipo iwe ukukumana ndi ine ndizida ndi nkondo. Koma ine ndikukumana ndi iwe mu Dzinala Ambuye Mulungu, ndipo lero ine ndichotsa mutu wako pamapewa ako.” Ndipo iye anachita zimenezo, chifukwa wamkulu

Page 44: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

44 MAWU OLANKHULIDWA

anali Iye amene amamudzodza Davide kuti alimbemtimachomwecho.194 Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu, kuposa chikukuchimenecho. Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu, kuposamachirawo. Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu, kuposa khansaimeneyo. Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu, kuposa chosautsachimenecho. Wamkulu ali Iye, kuposa chirichonse chimenechiripo chimenemdierekezi akhoza kuchiyika pa inu. “Wamkuluali Iye amene ali mwa inu, kuposa iye amene ali mdziko.”Wamkulu ali Iye! Inde!

Wamkulu anali Davide, chimene chinali mwa Davide;Mulungu mwa Davide.195 Iye ali mwa ife, ameneyo, ndi Khristu. Iye anali mgonjetsiwa mdani aliyense, wa ife. Pamene Iye anali kuno pa dzikolapansi, Iye anagonjetsa tchimo, Iye anagonjetsa matenda, Iyeanagonjetsa imfa, Iye anagonjetsa gehena, Iye anagonjetsamanda, ndipo tsopano Iye akukhala moyo mwa ife ngatiMgonjetsi! Iye anagonjetsa matenda, gehena, imfa, manda,ndipo anabwera kwa ife kuti adzatimasule ife ku zinthu zonsezimenezo. Ndipo wamkulu ali Iye amene ali mwa inu, kuposaiye amene angaike zonyenga izi pa inu. Inde! “Wamkulu ali Iyeamene ali mwa inu, kuposa iye amene ali mdziko.”196 Umo ndi mmene zozizwitsa izi zimachitikira. Umo ndimmene mphepo ija inasiyira, tsiku lina lija. Kodi munthuangachite zimenezo? Ayi, bwana, ndi zosatheka. Pameneine ndinaima pamenepo, ndikulira, ndipo mphepo zimenezozikukhadzula, ndipo…

Kodi ndi angati amene ali muno, amene analiko kumeneko?Tiyeni tiwone inu mukukweza manja anu. Kwezani manja anummwamba, aliyense amene anali kumeneko, kuntunda uko kuColorado nthawi imeneyo pa—pa nthawi imeneyo. Chabwino.M’bale Fred, ine ndikuganiza, ndi yekhayo amene analipo,pamenepo. Ine ndimaganiza mwinamwake M’bale Mann analipano, koma iye…M’bale, M’bale Evans, sanali iye? M’baleEvans anali kumeneko pa nthawi imeneyo. Eya. Chabwino.Ndipo, Eya.197 Zindikirani. Kodi izo si zoona? Kodi umo si mmeneizo zinachitikira? Mvula inangosiya, ndipo mphepo inasiyakuwomba. Kodi chinali chiyani icho? Pa mawu anga? Ayi!Chifukwa Iye anandiuza ine kuti ndichite icho. Ndipo wamkuluali Iye amene ali mwa ife, kuposa chirengedwe chirichonse.Kodi ameneyo si Mulungu yemweyo amene anakhoza kuimitsamafunde pa nyanja, anapangitsa mphepo kubwerera ku maloake? Kodi Iye si Yemweyo amene anadetsa dzuwa, anapangitsadzuwa liwale? Chabwino, “Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu,kuposa iye amene ali mdziko.”Mukuona? Chabwino.

Page 45: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 45

198 Tsopano ndi chifukwa chake zozizwitsa zoona izi zikhozakuchitika, chifukwa ilo ndi lonjezo la Mulungu, “Zinthu zimeneIne ndikuchita, mudzachitanso inu.” Yohane Woyera 14:12. Iye,Khristu, yemwe anapangitsa bata mphepo ndi mafunde, ndiMlengi wa izo. Iye akadali mochuluka panobe Mlengi mongaIye anali nthawi imeneyo. Iye ali yemweyo dzulo, lero, ndikwanthawizonse.

Iye anachiritsa odwala ndi kuwononga tchimo, ndipoanasintha zonsezo chifukwa cha inu, ndipo anabwera kwa inukuti Iye adzathe kukhala ndi inu. Iye anagonjetsa zonsezi,kuti adzabwere ndi kudzakhala mwa ife. Iye ndi Mgonjetsiameneyo amene anagonjetsa kale zinthu izi; anazitsimikizira izomuMalemba, anabwereranso ndipo anadzagonjetsa chirichonse,ndipo anatsimikizira kwa inu kuti Iye ali Mulungu yemweyo.Ndipo zitatha zaka naintini handiredi, pano Iye akuchitabechinthu chomwe chomwecho pakati pathu chimene Iye anachitanthawi imeneyo, amene anagonjetsa imfa, gehena, matenda, ndimanda!199 Khristu uyu, uyu “Iye,” Iyeyo ndi Iye amene ali mwa inu.Iye ndi Khristu. Monga Yohane ananena, “Iye amene ali mwainu ndi wamkulu kuposa Iye amene ali mdziko.” Ameneyo analiKhristu! Iye ali wamkulu kuposa dziko lonse chifukwa Iyeanagonjetsa dziko lapansi, ndipo iye ndiye wamkuluyo, kuposazinthu zonse izi, chifukwa Iye anatigonjetsera ife izo. “Ndipo ifendife oposa agonjetsi kudzera mwa Iye amene anatikonda ifendipo anadzipereka Yekha chifukwa cha ife,” kuti Iye adzathekubwereranso ndi kudzachita ntchito Zake kudzera mwa ife,kudzatsimikizira kwa ife kuti Iye ali yemweyo dzulo, lero, ndikwanthawizonse.

Pamene Iye anali pa dziko lapansi, Iye anatsimikizirapamene Iye anaima pakati pa anthu, Iye anali Mesiya. Iyeamatha kuzindikira maganizo amene anali mmitima mwawo.Ndipo Baibulo linati, Mose anati, kuti, “Iye akanadzakhalamneneri.” Nkulondola uko? Iye amadziwa zobisika za mumtima.Iye amadziwa amene anthuwo anali. Iye amadziwa chimenechinali chovuta ndi iwo. Kodi ife taziwona zimenezo zikuchitika?[Osonkhana akuti, “Ameni.”—Mkonzi.] Nthawi ndi nthawi!200 Ife tikudziwa kuti akufa adzutsidwa, kuchokera kwa akufakumene. Ena a iwo akhala atafa kwa tsiku ndi theka.Chabwino, anafa m’mawa wina, ndipo iwo nkumubweretsaiye usiku umenewo, ndipo anayenda usiku wonse; ndipotsiku lotsatira chaku masana, kapena madzulo pang’ono, iyeanabwera kumene msasa unali. Khanda laling’ono lakufa,litazizira, ndipo likugona mmikono mwa amayi ake. NdipoAmbuye Mulungu anamubweretsanso, anayankhula Mawu aMoyo, ndipo khanda limenelo linatenthetsedwa ndi kuyambakulira; nkumubwezeretsanso iyemu nkonowa amayi ake.

Page 46: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

46 MAWU OLANKHULIDWA

201 Akazi a Stadklev, ataima pamenepo akuwona izozikuchitidwa, ndi chifukwa chake iwo analira chomwechochifukwa cha khanda lawo, amafuna kuti ine ndiulukire kuGermany. Koma Ambuye anati, “Limenelo ndi dzanja Langa;iwe usachidzudzule icho.”Mwaona, inumukudziwa bwinoko.

Pamene Iye anamuuza Mose, anati, “Yankhula kwathanthwe,” usalikanthe ilo. Chimenecho chimatanthauza“yankhula,” usalikanthe, mwaona. Iwe umayenera kumverachimene Iye akuti uchite. “Koma palibe munthu angachitekalikonse mwa iyeyekha,” iye akuyenera kuti amve ichopoyamba kuchokera kwaMulungu.202 Tsopano Mawu a Mulungu analonjeza kuti Iye ali moyo.Ndipo, chifukwa Iye ali moyo, inu mudzakhala moyo. Iyeanalonjeza, kuti, “Ntchito zimene Ine ndikuchita inunsomudzazichita. Zinthu zomwe zomwezo, kungoti zochulukirapoza izo, inumudzazichita, chifukwa Ine ndikupita kwaAtate.” Iyeanagonjetsa zinthu zonse. Iye ndi Amene anaimitsa…

Iye ndi Amene anapanga agologolo aja. Zimenezozinachitika kawiri. Zinachitika kamodzi ku malo ako, Charlie.Ndipo izo zinadzakachitika—izo zinadzakachitika kuntundakuno pamene, abale, M’bale Fred ndi M’bale Banks ndi iwoanali uko ndi ife.203 Izo zinachitika ku Germany, pamene asing’anga fifitini aja,kumbali iliyonse ya ine, anati…Chifukwa Billy ndi M’baleArganbright sakanawalola iwo—iwo andiwone ine, iwo anati,“Chabwino, ife tipangitsa msasa uwo kusasukapo.” Ndipo iwoanakhala pansi pamenepo, ndi matsenga awo, ndipo anaitanirapa mulungu wawo, mdierekezi, ndipo apa iye anabwera ndinkuntho. Pafupifupi achi German sate sauzande, forte sauzandekumeneko, ndipo tenti imeneyo ikungonyamuka mmwamba ndipansi monga chonchi.

Iwo, ndipo kenako anadula, anatenga sizasi ndipo anadulanthenga, ndipo anailozetsa iyo mmbuyo monga choncho.Ndi kumanena zawozo, kumadutsa matsenga awo onse, ndikumanena mawu atatu oyera amene iwo amanena, “Atate,Mwana,MzimuWoyera; lu-lu-lu-lu-lu-lu! Atate,Mwana,MzimuWoyera; lu-lu-lu!”204 Kumapita monga choncho, ndipo ndithudi nkunthounabwerapo. Zedidi. “Iye ndi kalonga wa zimphamvu za mumlengalenga,” Satana. Ndipo iwo anaitanitsa nkunthowo.Ndipo, tsopano, ngakhale tenti yaikulu kwambiri ija itakhalapamenepo monga choncho, oh mai, iyo ikhoza kuphimbapafupifupi chimdadada cha mu mzinda; ndipo iyo itamangidwa,inamangidwa ndi ma thuu bai foro, ndipo basi chinsaluchitakhomedwa pamwamba pa icho. Mphepo inalowa pansipamenepo ndipo inangodzanyamula iyo, monga choncho. Ndipo

Page 47: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 47

mphepo imeneyo, ndi mphenzi zikung’anima monga choncho,ine ndimangopitirira kulalikira.205 Ndipo, oh, iwo amangopita mu kuwombeza kwakukulu,kumapitirira ndi kumapitirira monga choncho, akunena mawuaang’ono oyera awo amene iwo amanena, “Mawu atatuapamwamba oyera: Atate,Mwana, ndiMzimuWoyera,” kumbaliziwiri zonse monga choncho. Kenako ine ndinamuwona iyeakuwerama, ndipo atazunguliridwa ndi adierekezi pamenepo,koma osamangidwa.206 Ndipo ine ndinatiM’bale Lowster, “Musatanthauzire izi.”207 Ine ndinati, “M’bale Arganbright, mungopemphera.”208 Ine ndinati, “Ambuye Mulungu, Mlengi wa miyamba ndidziko lapansi, Inu munandituma ine kuno. Ine ndinapondetsaphazi langa pa nthaka iyi yaku German, mu Dzina la YesuKhristu, chifukwa Inu munandituma ine kuno. Mtamboumenewo ulibe mphamvu pa ine. Iwo ulibe, chifukwa ndinewodzodzedwa ndipo ndatumizidwa kuno chifukwa chachipulumutso cha anthu awa.”

“Ine ndikukulamulira iwe, mu Dzina la Yesu, kuti uchokepano.”209 Ndipo mabingu, akupita, “Bang’i! Bang’i! Bang’i!” Anapita,“Gruuuuuuuu,” akugudubuzika, ndipo molunjika pamwambapomwe pa tenti, inawomberanso mmbuyo; ndipo dzuwalinadzawala.210 Mkatikati mwa maminiti teni, apo panali pafupifupi tenisauzande atazungulira maguwa ndi zinthu, akufuula kufunachifundo, atawona mphamvu ya Mulungu. Chifukwa chiyani?“Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu, kuposa iye amene alimdziko.” Mukuona?211 “Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu, kuposa iye amene alimdziko.” Mukuona zosautsa mu chinthucho, oh, m’bale, mlongo,ife sitikuyenera kukhala ndi nkhawa iliyonse nkomwe. Ukuluwondi Mulungu, ndipo Iye ali mwa inu. Kodi inu mukukhulupirirazimenezo? [Osonkhana akuti, “Ameni.”—Mkonzi.]212 Tsopano ine ndadutsitsa nthawi. Ndi maminiti fifitini,pafupifupi, kudutsa naini. Ndipo ine ndikudziwa anthu awa alindi ulendo wautali woti ayendetse.

Tiyeni tiweramitsemitu yathu kwamphindi chabe.213 O Atate Mulungu, Inu mukudziwa za Colorado. Inumukudziwa zinthu zimenezo ndi zoona. Ndipo ine ndikunenaizo kwa ulemelero Wanu, kuti anthu awa akakhoze kudziwa.Zitatha zotsimikizira zonse za sayansi, za zithunzi, ndi zantchito ya Mzimu Woyera. Ndipo, Ambuye, Inu mukudziwa kutiIye…kuti ine ndanenamosabisa kwa anthu, ndipo nthawizonsendimatero, kuti ndi chifukwa chakuti Inu munalonjeza izi.Ndipo Inu muli pano, kuyesera kuti mupeze winawake amene

Page 48: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

48 MAWU OLANKHULIDWA

Inu mungadzitsimikiziremo Inumwini, kuwalola ena kuti awonekuti Inu muli wamoyo, ndipo Inu muli yemweyo dzulo, lero,ndi kwanthawizonse. Ine ndikukupemphani Inu, Ambuye, kutimutichitire chifundo, ndi kutitsogolera ndi kutilondolera ife mumaganizo athu.214 Pali iwo akhala pano amene akudwala ndi osautsika. Paliiwo amene mwina akhoza kufa ngati iwo sapeza thandizokuchokera kwa Inu. Ambiri a iwo, mwina, ali pa mapetoa ulendo, pamene madokotala sangawathandizenso nkomwe.Inu ndinu Mulungu, ndipo Ndinu yemweyo dzulo, lero, ndikwanthawizonse. NdipoKukhalapoKwanu kuli pano.215 Ndipo, Ambuye, ife sitikudziwa chimene ChikokaChachitatu ichi, monga ife talozera kwa Icho, chidzakhale. Inesindikudziwa chiyani. Koma ife tikudziwa chinthu chimodzi,kuti Chikoka Choyamba chinali ungwiro. Chikoka Chachiwiri,pokhala cha chisanu, chinali chisomo.

Ndipo, Mulungu, ine ndikupemphera usikuuno kuti Inumudziulule Nokha kwa ife, kuti zikatha zinthu izi, zakuti,“Iye amene ali mwa inu!” Ndipo Inu munati, “Ntchito zimeneIne ndikuchita kuti inunso mudzatero,” ndipo munati Inusimumachita kanthu kufikira Atate atakuwonetsani Inu.216 Ndipo ife tawona zimene Inu munachita pamene Inumunatha kumuwuza Mtumwi Petro yemwe iye anali, chimenedzina la abambo ake linali. Munamuuza Natanieli chimenentchito yake inali, mmene iye anadzafikira pamenepo, kumeneiye anali asanafike, chimene iye amachita. Munamuuza mkazi,pa chitsime, za machimo ake ndi chimene iye anali, kukhalamu chigololo ichi ndi amuna asanu ndi m’modzi awa; asanuanali atakhala nawo, ndipo m’modzi amene iye amakhalanaye tsopano sanali mwamuna wake. Inu mukadali Mulunguyemweyobe. Inu munamuuza…217 Chinali chikhalidwe cha khungu cha Bartumeyo, pameneiye anaima pamenepo; komabe, mu mtima mwake, iye anali ndikupenya, kuti iye amakhoza kuwona; kuti, ngati ameneyo analiYehova akuwonetseredwa mu Umwana wa Yesu Khristu, kutiIye anali wokhoza kudziwa kufuula kwake. Ndipo iye anafuulamokweza, “Inu Mwana wa Davide, ndichitireni ine chifundo!”Ndipo izo zinakuimitsani Inu, ndipo Inu munapotoloka ndipomunamuchiritsa iye, O Atate, kumuuza iye kuti chikhulupirirochake chinali chitamupulumutsa iye.218 Mkazi wamng’ono wochepa magazi uja, kuti kudzera muvuto la magazi ili ndi kusinthika kwa moyo, ndipo kwa zakazambiri iwo samasiya. Iye anali atataya ndalama zake zonse kwamadokotala, ndipo panalibe aliyense wa iwo amamuthandizaiye. Iye anabwera ku umodzi wa misonkhano Yanu pameneInu mumayankhula kwa munthu kumeneko ku—ku Galileya,pamene Inu munali pa ulendoWanu wopita ku nyumba ya Yairo.

Page 49: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 49

Mkaziwamng’ono uyu anali atanenamumtimamwake, popandaLemba kumbuyo kwa izo, “Ngati ine nditangokhoza kukhudzachovala Chake, ine—ine ndikukhulupirira kuti ine ndikhalabwino.” Ndipo iye analandira chokhumba chake pamene iyeanadzakhudza chovala Chanu. Ndipo Inu munamuuza iye kutichikhulupiriro chake chinali chitachita izi, chinafotokozerazofuna zake, ndipo iye anachiritsidwa.219 Ife timauzidwa mu Mawu kuti Ndinu WansembeWamkulu, amene mukukhala Mmwamba, nthawizonse wamoyokuti muzipanga chitetezero. Ndipo—ndiponso kuti Inu,pokhala Wansembe Wamkulu, pa nthawi ino, amene akhozakukhudzidwa ndi zomverera za zifooko zathu. AmbuyeMulungu, mupereke kuti munthu aliyense pano usikuunoathe ku…akhale nawo mwayi wokukhudzani Inu usikuuno,Wansembe Wamkulu wopambana, ndipo achiritsidwe. KwaUlemelero wa Mulungu, ine ndikupempha izi mu Dzina la Yesu.Ameni.220 Tsopano ine sindiku…Kodi pali makadi a pemphero? Ine—ine ndinamuuza Billy osati…kodi aliyense ali ndi makadia pemphero? Chabwino, uko nkulondola, ine ndinamuuzaiye kuti asapereke iwo. Ine ndimaganiza kuti mwina inenditalikitsa pang’ono, pamene ine…oh, ine ndimangoyankhulakwambiri. Koma, yang’anani, taonani, ndipo inu munandiuzaine, pamene ine ndinati, “Ine ndiyesetsa kuti ndituluke pofikahafu-eyiti,” inu munaseka, ndipo ine—ine ndinadziwa kuti inumumadziwa chimene inumumakamba. Ine—ndine…koma ine—ine ndimakukondani inu. Mukuona?221 Chiyani, chimene ine ndikuyesera kuti ndichite, inenthawizonse ndayeserapo ichi, mzanga; palibe kuti wina aziti,“M’bale Branham anachita ichi.” M’bale Branham sangathekuchita chirichonse. Mukuona? Ndi Yesu Khristu. NdipoIye amene ali mwa ine ali mwa inu. Inu mukungosowa kutimukhulupirire. Kodi si kulondola uko? Mukuona? Iye amene alimwa inu ndi wamkulu kuposa nthenda yanu.222 Tsopano ndi anthu angati muno amene akudwala mmatupiawo, simukundidziwa ine, koma inu mukukhulupirira kutiinu muli ndi chikhulupiriro chokwanira kuti mumukhudzeWansembe Wamkulu, kwezani m’mwamba dzanja lanu, mukuti,“Ine ndikukhulupira izo”? Chabwino. Oh, pafupifupi paliponse,pali manja. Chabwino. Ndi angati muno amene akundidziwa ine,ndipo akudziwa kuti ine sindikudziwa kanthu za chimene inumukuchisowa, ndipo inu mukufuna Mulungu kuti akukhudzeniinu? Kwezani m’mwamba dzanja lanu. Mukuona? Mukuona?Chabwino.223 Moona, palibe aliyense muno amene ine ndikudziwachirichonse chake, pompano pa nthawi ino, za kukhalawodwala.Koma mnyamata uyu wakhala apa, ine ndikumudziwa iye.

Page 50: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

50 MAWU OLANKHULIDWA

Ine ndamupemphererapo iye, nthawi zambiri. Ine ndikulepherakuganizira dzina lake, koma iye ndi wochokera kumusi kuKentucky. Iye amandilembera ine nthawi zonse, bwenzi lakelakelaM’bale ndi MlongoWood ndi iwo, ndipo amabwera kumeneko.Ndipo iye wakhalapo pamisonkhano kwa nthawi yaitali, nthawiyaitali. Ameneyo ndimunthu yekhayo ine ndikumudziwa.224 Tsopano, M’bale Dauch, mmene ine ndikudziwira, ali bwino,kapena iye sibwenzi atakhala pano. Iye anadwalika kwambiritsiku lina, ndipo Ambuye anamuchiritsa iye.225 Ine sindikumudziwa munthu uyu. Ndipo inesindikumudziwa kuti uyo ndi ndani amene ali ndi ndodoizi apa; mwinamwake bambo uyo ali mchikuku. Ine—inesindikumudziwa.

Ndipo ine—ine ndikudziwa ambiri a inu. Koma MulunguKumwamba akudziwa, pa nthawi ino, ine sindikudziwa chimeneinumukufuna. Ine ndiribe lingaliro. Zimakhala ngati zovutirapokuno ku kachisi, chifukwa, onani, ine ndimadziwa anthu ambiri.226 Tsopano ndi ichi chimene chiri. Pamene iwe ufika pamalo…Tsopano, ine ndimabwera kuno, nthawizina, ndipo inendimati, “Chabwino, ife timupatsa aliyense khadi la pempherondipo nkuwafoletsa iwo. Bwerani pa nsanja.” Winawakeamachokapo…Tsopano iwe sungathe…

Tsopano, abwenzi, ine nditsegula mtima wanga ndipondikuuzani inu chinachake. Inu simungabise zimenezo. Basizimene inu mukuganiza, ine ndikuzidziwa izo. Uko nkulondola.Ine ndikudziwa zimene inu mukuganiza. Mukuona? Ndiponthawizina inu mumati, “M’bale, ine ndikukhulupirira.”Bwanji, chabwino, inu mumakhulupirira kufikira ku mulingo.Mukuona? Mukuona? Ine ndimadziwa.227 Ndipo pomwe pano, pamene ine, pakali pano, kudzodzakukungobwera pa ine, inu mwaona. Ndipo ine ndikuthakumverera kututuma kumeneko, ngati, kugunda, mwaona,kugundagunda kuchokeramalo osiyanasiyana.Mukuona?

Koma tsopano musati—musati muzikaikira nkomwe.Mukhulupirire Uthenga wonse. Mukhulupirire Iwo. Ngatisi choncho, ngati izo sizinalembedwe mu Baibulo, ndiyeinu musazikhulupirire izo. Koma ngati Izo ziri mu Baibulo,ndiye Mzimu Woyera umene ukukhala moyo mwa ife ndiwokakamizidwa kuti uchite zimenezo ngati ife tikhulupirira Izi.Nkulondola uko? [Osonkhana akuti, “Ameni.”—Mkonzi.]

Ine ndikudziwa izo ndi zovuta. Mwaona, palibe chimenechimabwera mophweka.228 Izo zinali zovuta kwa Iye kuti afe, kuti ichi chikhozekuperekedwa kwa inu. Zinali zovuta kuti Iye apite ku Kalvare;Iye ankafuna kuti akhale, ngakhale mochuluka kwambirikufikira kuti Iye analira, “Osati kufuna Kwanga, koma Kwanu

Page 51: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 51

kuchitidwe.” Mukuona? Mukuona? Iye sankafuna kuti achoke;Iye anali Munthu wachichepere, ndipo Iye anali ndi abaleAke. Iye ankawakonda iwo chimodzimodzi basi monga inendimakukonderani inu. Koma Iye—Iye sakanatha kukhala ndimoyo, ndipo iwo nkukhalanso ndi moyo, chotero Iye anafakuti ife tidzathe kukhala ndi moyo. Chimenecho sichinalichophweka. Iye ankayenera kuti achite icho. Taonani imfaimene inali patsogolo pa Iye, “Atate, ora lafika, ndipo kodi Inendipemphere kuti Inu mundichotsere chikho ichi kwa Ine? Ayi.”Iye sanafune kuti achite zimenezo; Iye ankafuna chifuniro chaMulungu kuti chichitidwe.229 Tsopano, taonani, ngati inu muti mukhulupirirechinthu chomwe chomwecho! Tsopano, musati—musati—musachiphimbe Icho, nkomwe. Mungochikhulupirira icho.Mwamtheradi mungochikhulupirira icho. Musakaikire. Inumukhulupirire icho.230 Ngati ine ndiwabweretsa anthu mu mzere wa pemphero,ndipo ine nkuti, “Chabwino, tsopano munthu uyu, inumukudziwa ine sindikukudziwani inu.”231 “Ayi, uko nkulondola, M’bale Branham.”232 Ndiye pomwepo apo iwe umamupeza wina akuti, “Uh-huh,koma iye akuwerenga zimene iwo alemba pa khadi la pempherolimenelo!Kuwerengamaganizo!” Izo ndithudi zimachita izo.233 Ndiye ine nkuti, “Chabwino, tsopano Lamlungu ili ifesitipereka makadi a pemphero aliwonse. Ine ndikufunaaliyense pano, amene ali mlendo, sanakhalepo muno nkalelonse, inu muimirire.” Mukuona? Ndipo—ndiyeno MzimuWoyera nkupotoloka ndipo nkuzindikira zonse zimene zinalimwa iwo. Mukuona? Nkulondola uko? [Osonkhana akuti,“Ameni.”—Mkonzi.] Inumunaziwonapombali ziwiri zonsezo.234 “Oh, chabwino, pali chinachake cholakwika ndi zimenezo.”Mukuona? Mukuona? Apo, palibe njira iliyonse, inu—inu—inusimungathe…Mwaona, bola ngati Satana angakugwireni, iyebasi adzakupangani inu kukhulupirira chirichonse.

Ndipo iye akuwonetsani inu cholakwika chirichonsechimene ine ndiri nacho, ndipo ine ndiri nazo zochuluka za izozimene iye angathe kukuwonetsani inu. Inu musamayang’anepa izo! Inu musamayang’ane pa izo. Ndine munthu. Mukuona?Koma, kumbukirani, Mawu awa aMulungu ndi Choonadi, ndipoine ndikuyesera kukhala moyo ndi Iwo.235 Ngati ine nditamapita uko ndi kumakayamba kuchitazinthu molakwika, zomwe ziri zolakwika, kumachimwa, ndikumamwa, ndi, kapena kumasuta, kapena—kapena kumachitazinthu zimene siziri zabwino, inu—inu mubwere ndipomudzandiitanireko ine, chifukwa izo—izo si zabwino. Ine—inendikufuna zitatero ndichoke pa dziko lapansi. Ine sindingati…

Page 52: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

52 MAWU OLANKHULIDWA

Ine ndikufuna kudzachoka izo zisanachitike. Mukuona? Inesindikufuna kudzachita zimenezo.236 Koma ngati ine ndikuyeserabe kukhala moyo wachimene chiri chabwino ndi kuchita chimene chiri chabwino,mwaona, ndi kuyesera kumakhala monga Mkhristu ayenerakuchitira, ndiyeno nkumulola Mulungu kuti atenge MawuAke ndi kumandimva ine ndikuima ndi Iwo. Ngakhale Iwoatandichotsera ine abwenzi ambiri ndi kutchuka kwa mdziko,ndi zinthu monga choncho, ndi kudedwa ndi ambiri, ndizipembedzo, kutulutsidwa panja, komabe ine ndikufunandikhale woona ku Mawu awa. Iwo ndi Mawu a Mulungu, ndipoine ndimamukonda Mulungu. Chotero ndi Mawu a Mulungu,ndipo ine—ine ndikukuuzani inu kuti, “Iye ali yemweyo dzulo,lero, ndi kwanthawi zonse,” ndipo Iye ali mwa ife tsopano. Ndipongati chi…237 Tsopano, ngati moyo wa Shakespeare ukanamakhalamwa ine, kumakhala moyo mwa ine, ngati Shakespeareakanamakhala moyo mwa ine, kodi ine sibwenzi ndikuchitantchito za Shakespeare? Ngati Beethoven ali mwa ine, kodiine sibwenzi ndikuchita ntchito za Beethoven? Ngati mzimuwa Dillinger ukanamakhala mwa ine, ngati John Dillingerakanamakhalamwa ine, kodi ine sindikanakhala JohnDillinger?Ngati Beethoven akanamakhala mwa ine, ine ndikanakhalaBeethoven? Mukuona? Ngati Castro akanamakhala mwa ine, inendikanakhala Castro? Mukuona?

Ndipo ngati Yesu Khristu ali mwa ine, ntchito Zake inendizichita, chifukwa akhala Iyeyo. Ndipo kodi Iye sananenekuti chinthu chomwecho chidzachitika? Mukuona? [Osonkhanaakuti, “Ameni.”—Mkonzi.]238 Tsopano kodi Iye akanachita chiyani ngati Iye akanatiwaima pano, ngati Iye ali yemweyo dzulo, lero, ndikwanthawizonse? Iye akuti, “Ine ndikhoza kokha kuchitachimene Atate andisonyeza Ine kuti ndichite.” Nkulondola uko?Chabwino, ndi mmene Iye anachitira izo dzulo.

Tsopano kodi Iye ali yemweyo? Nanga bwanji nthenda?Mtengo wanu unalipiridwa kale. Aliyense wa inu wachiritsidwakale nthenda yanu. Nkulondola uko? [Osonkhana akuti,“Ameni.”—Mkonzi.] Pakuti icho…Aliyense wa inuwakhululukidwa, koma inu mukuyenera kuvomereza izo.Aliyense wa inu wachiritsidwa, koma inu mukuyenerakuvomereza izo.239 Tsopano, pofuna kutsimikizira kuti Iye ali yemweyo dzulo,lero, ndi kwanthawizonse. Ngati Iye akanati waima pano, Iyesakanakuchiritsani inu, nkomwe, ndi kusakhulupirira kwanuko.Inu mukanayenera kuti mukhulupirire izo, chimodzimodzibasi mmene inu mukuyenera kukhulupiririra izo pakali pano.Izo zikuyenera kukhala chimodzimodzi, mwaona. “Chifukwa,

Page 53: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 53

ntchito zambiri zamphamvu Iye sanathe kuzichita mu tsikuLake, chifukwa cha kusakhulupirira kwawo.” Kulondola uko?Ntchito zamphamvu zambiri Iye akulephera kuzichita lero,chifukwa cha kusakhulupirira.240 Tsopano, Ndi ndani amene amatha kulosera izo? Mulungu.Ndi ndani amene ananena izi? Mulungu. Ndi ndani ameneanachita izo? Mulungu. Ndi ndani amene ananena kumenechimbalangondo, gwape, mphalapala, zinthu zina zonse izi, ndizisanu ndi ziwiri…zonse—zinthu zonse izi zimene zachitika?Ndi ndani amene ananena zimenezo? Iye, Khristu, amene alimwa ife, kudzinenera Yekha kudzera mwa ife, kudziulula Yekhakuti Iye ali yemweyo dzulo, lero, ndi kwanthawizonse.

Nndani anaimitsa mphepo? Nndani analenga agologolo?Yemwe Uja amene analenga mwanawankhosa kwa Abrahamu,pamene iye…anamutcha Iye “Yehova-yire.” Maina apawiria chiombolo awo akugwirabe ntchito pa Iye. Iye akadalipanobe Yehova-yire, “Ambuye akhoza kudziperekera IwowokhaNsembe.”241 Tsopano, aliyense wa inu, ine—ine ndikufuna kuwonamtima kwanu kwakuya tsopano. Ngati inu mungakhulupirirekwenikweni ndi mtima wanu wonse, sipakhala munthu wofookapakati pathu, pamene wotchi iyo izizungulira maminiti enafaifi. Sipakhala munthu pano koma amene akhale ataimirira pamapazi ake, alibwino, ngati inu mutangokhulupirira izi. Kodiinu mungakhulupirire?242 Tsopano tiyeni tingowona tsopano ngati Iye angabwerekwa ife ndi kudzadziulula Yekha, pamene ife tikuweramitsamitu yathu.243 Ambuye Yesu, tsopano Inu mundithandize ine. Ndipo inendikumverani Inu, Ambuye, zonse zimene ine ndikuzidziwakutero. Khululukirani machimo anga ndi kulakwitsa. Inendikupemphera muDzina la Yesu. Ameni.244 Tsopano tiyeni titenge mbali iyi apa, winawake uku.Khulupirirani, mukhale ndi chikhulupiriro, musati mukaikire!Winawake amene sakundidziwa ine, ngati nkotheka.Ine sindinganene kumene masomphenya akupita. Inendikungoyenera kuchipenyerera Icho. Ndipo ngati Icho chichitazimenezo, ndiye inu mudziwa izo, ngati ziri zoona kapenaayi. Inu mungokhulupirira, ndipo musakaikire. Ngati Iye atiachite izo, kodi inu mukhulupirira, mwaona, zitatha zonseizi zimene zachitika lero? Mukuona? Ingolandirani machiritsoanu, mwaona. Munene, “Ambuye, ine tsopano ndikumukhudzaYesu Khristu. Ine ndikukhulupirira.” Tsopano Mulungu waKumwamba apereke izi.245 “Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu, Khristu, kuposaiye amene ali mdziko.” Tsopano, mu msonkhano, kumene ifetimamukhudza Iye, Iye akudzinyezimiritsanso Yekha; monga

Page 54: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

54 MAWU OLANKHULIDWA

mkazi anamukhudzira Mulungu, kudzera mwa Khristu, ndipozinanyezimiritsanso zosowa zake.246 Ine ndikuwona tsopano pa ngodya apa, akuwoneka ngati ndimwamuna, iye wadwalika kwambiri. Ayi, si choncho. Ndi mkaziakumupempherera mwamuna, ndipo mwamunayo sali pano.Koma ndi mkazi. Ine ndikuwona kuti mkazi ameneyo…Ndiake—bambo ake, ndipo iwo akufa ndi khansa. Ndipo adwalikakwambiri. Bamboyo sali pano. Iye ali ku malo ena. Si dziko lino,nkomwe. Ndi, iye ali ku Georgia.

Ingopitirirani kupemphera. Inu mukhulupirire ndi mtimawanu wonse tsopano? [Osonkhana akuti, “Ameni.”—Mkonzi.]Zipitirirani kupemphera, mwaona.

Dzina la mkaziyo, akupempherayo, ndi Akazi a Jordan.Iye si wochokera ku Georgia. Iye ndi wochokera ku NorthCarolina. Ngati uko nkulondola, dona, imirirani pa mapazianu. Kulondola, zonse zoona. [Mlongoyo akuti, “ZikomoMulungu! Zikomo Mulungu!”—Mkonzi.] Munali inu amenemmapempherera zimenezo? [“Inde, bwana; adadi anga.”]Chabwino. Chabwino. [Mlongo akupitirira kuchitira ndemangaza abambo ake.]

Kodi inu mukukhulupirira, kuti, “Iye amene ali mwa inundi wamkulu kuposa iye amene ali mdziko”? [Mlongoyo akuti,“Ine ndikutero.”—Mkonzi.] Kodi inu mukukhulupirira kuti Iyeamene…247 Tayang’anani, apa pali chinachake. Inu mwakhalapondi kuphunzitsidwa kwakukulu mmasiku anu oyambirira,kapena chinachake chimzake, chifukwa zikuwoneka ngati inumwasakanizika kapena mu mtundu wina wa Mkhristu…Kodi bambo anu si mtumiki, kapena winawake mongachoncho, ena a anthu anu, kapena chinachake? [Mlongo akuti,“Mwamuna wanga.”—Mkonzi.] Mwamuna wanu, ndi ameneiye ali. Ine ndikutha kumuwona winawake ataima pambalipanu, akulalikira Uthenga, ndipo inu munali mu tchalitchi. Iyewolumikizana ndi inu. [“Ambuye Alemekezeke!”] Chabwino,ndi zimenezotu.

Tsopano, donayu ine sindikumudziwa, koma Mulunguakumudziwa mkaziyu.248 Tsopano, kodi inu muli ndi chinachake mkathumba kabukhu, kampango kakang’ono kapena chinachake m’menemo?Chabwino, ndiye inu muk-…Pamene inu mukakhalapansi, mukaike manja anu pa kampango kameneko, ndipomusakakaikire, ndipo Iye amene ali mwa inu ndi wamkulukuposa iye amene akupha adadi anu. Mukhulupirire ndi mtimawanuwonse, chotero izo zikhalamonga inumukukhulupirira.249 Tsopano, ine ndikufuna kuti ndikufunseni inu chinachake.Ine sindikumudziwa mkazi uyo. Mmene ine ndikudziwira,imeneyi ndi nthawi yoyamba, ine ndikuganiza, ine

Page 55: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 55

ndinamuwonapo iye. Koma iye wakhala pamenepo muchikhalidwe chosimidwa, akupemphera. Ndipo Mulunguyemweyo amene anakhoza kupotoloka ndi kumuuza mkaziza vuto lake la magazi, ndi Mulungu yemweyo yemwe alipano, akusonyeza kuti Iye amene ali mwa inu wagonjetsadziko lapansi. Inu mukukhulupirira? [Osonkhana akuti,“Ameni.”—Mkonzi.] Ngati inu mungokhala ndi chikhulupiriro,musakaikire.250 Kukamba za khansa, ine ndikuwona mthunzi wakudauwo kachiwiri. Uli pa mkazi, wakhala pomwe apa. Iye alindi khansa ya pakhosi, ndipo iye ali mmawonekedwe oyipa.Ndipo iye wapemphereredwa, ndipo akuyesetsa kuti alandiremachiritso ake. Akazi a Burton, ngati inumungakhulupirire! Inesindikumudziwa mkaziyo. Koma ngati inu mungakhulupirirendimtimawanuwonse…Kwenikweni, chinthucho…

Ndiloleni ine ndifotokoze ichi kwa inu, chimene inumukuyesetsa kuti muchite. Inu mwataya mawu anu, chifukwacha icho, ndipo inu mukuyesetsa kupempherera mawu anukuti abwererenso. Nkulondola uko? Gwedezani dzanja lanumonga chonchi. Tsopano, mkaziyo ndi mlendo kwa ine. Inesindikumudziwa iye. Mwamuwona iye? Uko nkulondola. Apo,ndi uyo apo. Mukuona? “Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu,chikhulupiriro chimene chingamukhudze Iye, kuposa iye ameneali pakhosi panu.”

Inu mukukhulupirira ndi mtima wanu wonse? [Osonkhanaakuti, “Ameni.”—Mkonzi.]251 Mlongo Larsen, ine ndikukudziwani inu. Iye ndi mwiniwa nyumba yanga. Koma, Mlongo Larsen, inu mwakhala mulikwa dokotala kapena chinachake, chinachake chimzake. Inumukuyembekezera opareshoni. Uko nkulondola. Nkulondolauko?Wamkulu ali Iye amene alimwa inu,MlongoLarsen, kuposaiye amene ali mdziko. Yesu anati, “Ine ndinali mlendo, ndipo inumunandilowetsa Ine mkati. Mochuluka mmene inu mwachitirakwa aang’ono awa, aang’onoAnga, inumwachitira izo kwa Ine.”

O Atate a Kumwamba, tichitireni chifundo!252 Kodi inu mukuganiza chiyani? Inu mukuyembekezeraopareshoni, inunso. Ndinu mlendo kwa ine. Nkulondola uko?[Mlongo akuti, “Inde.”—Mkonzi.] Sindinu wochokera kuno.[“Ine ndikukudziwani inu, koma inu simukundidziwa ine.”]Inu mukundidziwa ine, koma ine sindikukudziwani inu.[“Inu simukundidziwa ine.”] Koma Mulungu amakudziwaniinu. Inu mukukhulupirira zimenezo? [“Inde, ine ndikutero.”]Inu mukuyembekezera opareshoni. Inu simumakhala kuno.Inu mwayandikira Bedford, Springville, chinachake ngati…Ndi kumeneko, Springville. Akazi a Burton…Ayi, ayi, inendikupempha kukhululukira kwanu, ine sindimatanthauzazimenezo. Akazi a Parker, dzina lanu ndi limenelo. Si

Page 56: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

56 MAWU OLANKHULIDWA

choncho? Wamkulu ndi Iye amene ali mwa inu, kuposa iyeamene akuyesera kuti akupheni inu. Nkulondola uko? Kodiinu mukukhulupirira ndi mtima wanu wonse? Ndiye inusimukasowa opareshoni yanu, ngati inumukutero.253 Kodi inu mukuganiza chiyani pa zonse izi, mlongo? Inesindikukudziwani inu. Ndinu mlendo kwa ine. Kodi inumukundikhulupirira ine kukhala mneneri Wake? [Mlongo akuti,“Ine ndikukhulupirira izi.”—Mkonzi.] Inu mukutero. Zikomoinu. Mulungu alemekeza chimenecho. Inu ndinu Akazi aWhite. Inu mumachokera ku Fort Worth, Texas. Inu muli ndinthenda ya minyewa, vuto la mitsempha. Inu simuli bwino.Palibepo chiyembekezo kwa inu, tikakamba za sayansi yazamankhwala. Amuna anu, ali ndi chosowa chauzimu chimeneiye akuchipempherera. Inu muli ndi mwana kumeneko, iye alindi vuto ndi nsana wake, ndi vuto la mtima. Inu muli ndimnyamata wamng’ono pa miyendo yake. Mnyamata wamng’onoameneyo ali ndi kayankhulidwe ka mtundu wina kamene inumukukapempherera. Ngati uko nkulondola, kwezani mmwambadzanja lanu. [Mwamunayo akuti, “Uko nkulondola. Ndizozosowa zathu.”]

“Wamkulu ali Iye amene ali mwa inu, kuposa iye ameneali mdziko.” Kodi inu mukukhulupirira zimenezo? [Osonkhanaakuti, “Ameni.”—Mkonzi.] Ndi mtima wanu wonse? [“Ameni.”]Ndi zonse za izo? [“Ameni.”]

Tsopano tiyeni tiweramitse mitu yathu.254 Tsopano Iye wadutsa mchipindachi. Iye watsimikizira kwainu kuti Iye ndiMulungu. “Wamkulu, uyu Iye amene ali mwa inu,kuposa iye amene ali mdziko.” Ndi Ambuye Mulungu. Tsopano,Iye amene ali mwa inu, muloleni Iye akhale ndi uyambiriro.Muloleni Iye akhale ndi chonenapo cha—cha chimene inu…

Inu munene mu mtima mwanu pakali pano, ngati inumungathe, ndi mtima wanu wonse, ndipo mukhulupirire ichi,“Nthenda imene inali mthupi mwanga yachoka.” Mukuona?“Ine sindisautsidwanso. Ine ndiribenso matenda. Iye amene alimwa ine ndi wamkulu kuposa iye amene ali mthupi mwanga.Iye amene ali mu mtima mwanga ndi wamkulu kuposa iyeamene ali mu mnofu wanga. Chotero, Iye amene ali mu mtimamwanga analenga miyamba ndi dziko lapansi. Mnofu wangawaipitsidwa ndi Satana, ndipo ndine kachisi wakuti MzimuWoyera azikhalamo. Chotero, Satana, ine ndikukulamulira iwekuti ulisiye thupi langa. Mu Dzina la Yesu Khristu, tuluka mwaine.” Mukuona? Inu mukukhulupirira zimenezo? [Osonkhanaakuti, “Ameni.”—Mkonzi.]

Tsopano tiyeni tonse tipemphere mwanjira yathu yathutsopano, mmodzi aliyense, pamene ine ndikukupemphereraniinu.

Page 57: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU 57

255 Mulungu Wamphamvuzonse, Mlengi wa miyamba ndidziko lapansi, Mwini wa moyo, Wowulula zinsinsi za mumtima, Inu munati, “Mawu a Mulungu ndi akuthwa kuposalupanga lakuthwa-konsekonse, ndipo ngakhale ndi Wozindikiramaganizo a mu mtima.”256 Ndi chifukwa chake, pameneMawu anasandulika thupi, Iwoanazindikira zimene iwo amaganiza, pamene Iye amazindikiramaganizo awo. Iye anali Mawu, ndipo Mawu amadziwa zobisikaza mitima yawo.

Ndipo Mawu amenewo akanali Mawu omwewo. Ndipousikuuno ife tikuwawona Iwo akudziulula Wokha mwa ife,patatha zaka thuu sauzande, chifukwa Iye anawalemba Iwo papepala ndipo ali pano kuwatsimikizira iwo, kuwawonetsera iwo,kuti Iwo ndi owona.257 Apa pali mipango yayalidwa apa. Anthu odwala aliponseponse. Ine ndikupemphera kuti Mzimu Woyera wawukuluumene uli pano, umene umasonyeza zinthu izi, umene umanenazinthu izi, ndipo sizilephera nkomwe, koma chimene chiricholondola, palibe nthawi imodzi Iwo ungalephere, chifukwaIwo ndi Mulungu. Mulole Iye adzodze mipango iyi ndiKukhalapo Kwake, ndipo achize munthu wodwala aliyenseamene iyo iti ikaikidwepo. Ndipo Mulungu Amene akhozakukhala wamoyo, patatha zaka thuu sauzande, ndipo akhozakuziumba Yekha mmitima ya ochimwa amene awomboledwamwa chisomo ndi chikhulupiriro, ndipo akhoza kuyankhulaMawu Ake Omwe kudzera mmilomo ya chivundi, ndiponkumaziwona izo zikuchitika ndendende basi zimene Iyeanalonjeza.258 O Ambuye Mulungu, ine ndikukupemphani Inu kutimutichitire ife chifundo. Ndipo mulole mwamuna aliyense ndimkazi amene wakhala pano, amene ali ndi mtundu uliwonse wamatenda kapena chosautsa; ndipo monga Mose anadziponyerayekha pa cholekanitsa, chifukwa cha anthu, usikuuno inendikuika mtima wanga pamaso pa Inu, Ambuye. Ndipo ndichikhulupiriro chonse chimene ine ndiri nacho, chimene chirimwa Inu, chimene Inu mwandipatsa ine, ine ndikupereka kwaiwo. Monga Petro ananena pa chipata chotchedwa Chokongola,“Chimene ine ndiri nacho, ine ndikukupatsa iwe. Mu Dzina laYesu Khristu wa ku Nazareti, dzuka ndipo uyende.” Ndipomunthuyo anali wolumala ndi—ndi wofooka kwa mphindipang’ono, koma, pamene iwo anamugwiriziza iye, mafupa apachidendene analandira mphamvu. Ndipo iye analowa Mnyumbaya Mulungu, akulumphalumpha, ndi kulemekeza ndi kudalitsaMulungu.259 Inu muli yemweyo dzulo, lero, ndi kwanthawizonse.Ndipo mtumwi Wake anati, “Chimene ine ndiri nacho, inendikukupatsa iwe.” Icho chinali chikhulupiriro. Ndipo ine

Page 58: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

58 MAWU OLANKHULIDWA

ndikuti: chimene ine ndiri nacho, ine ndikupereka kwaomvetsera awa! Mu Dzina la Yesu Khristu wa ku Nazareti,akaneni matenda anu, chifukwa wamkulu ali Iye amene alimwa inu, kuposa mdierekezi amene akuyesera kuti atenge moyowanu. Inu ndinu ana aMulungu. Inumuli owomboledwa.260 Ine ndikulamulira kuti Satana uwasiye anthu awa. MulunguAmene anabweza nkuntho uja tsiku lina, Mulungu Ameneanapangitsa mphepo ndi mafunde kuti zisiye, mulole Iyeawonetsetse kuti nthenda iliyonse yachotsedwa pa anthu awa,ndipo mphamvu ya Khristu ikuwonetseredwa mmoyo wawopa ora lino. Mulole wochimwa aliyense alape. Mulole munthualiyense, amene sali pafupi ndi Inu, akonzeke pa ora lino. Ndipomulole izo zikhale chomwecho,muDzina la YesuKhristu.261 Ine, ngati m’busa wanu, m’bale wanu, ndi chikhulupirirochimene ine ndiri nacho, ine ndamupempha Mulungu kutiachiike icho pa inu. Ine ndikukhulupirira kuti ine ndilandirachimene ine ndapempha. Tsopano ngati inu mungakhulupirireizo ndi ine; ndi chikhulupiriro chimene ine ndiri nacho, inendikupereka kwa inu chifukwa cha ora lino.

Ndipo tsopano, mu Dzina la Yesu Khristu, Mwana waMulungu, mukukane kusautsika kwanu, nthenda yanu, ndipomunene kwa izo, “Iwe uyenera kuti uzipita,” chifukwa inu mulindi chikhulupiriro chanu, kuphatikiza chikhulupiriro changa,ndi mphamvu ya Yesu Khristu, Amene kupezekaponseponseKwake kuli pano kuti kudzawonetsere izo ndi kudzatsimikizirakuti Iye ali pano, akuchizani inu pa nthawi ino.262 Kodi inu mukukhulupirira zimenezo, dona, mwagona pamachira awa? [Mlongo akuti, “Uko nkulondola.”—Mkonzi.]Ngakhale minyewa yanu yonse itakhala mmene iwoamazitchulira izo, phudzi ndi zinthu, inu mukhoza kuyendangati inu muti muyesere. Imirirani, mu Dzina la Yesu Khristu.Muthandizireni iye pamenepo. Ndi uyo pamenepo. Kodi inusimukukhulupirira? Ena nonse a inu, imirirani. Mafupa achidendene chake alandira mphamvu.

Tsopano tiyeni tikweze manja athu ndi kumpatsa Iyematamando.263 Yehova Wamkulu Mulungu, mu Dzina la Yesu Khristu,ife tikudzipereka tokha kwa Inu chifukwa cha machiritso.Ameni.

Page 59: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

IYE AMENE ALI MWA INU CHA63-1110E(He That Is In You)

Uthenga uwu wa M’bale William Marrion Branham unalalikidwa muChingerezi, Lamlungu usiku, Novembala 10, 1963, ku Branham Tabernacle muJeffersonville, Indiana, U.S.A. Unatengedwa kuchokera pa matepi ojambulidwandi maginito nudindidwa mosachotsera mawu ena mu Chingerezi. Kumasulirauku kwa Chichewa kunadindidwa mu chaka cha ndi Voice of God Recordings.

CHICHEWA

©2019 VGR, ALL RIGHTS RESERVED

VOICE OF GOD RECORDINGS, MALAWI OFFICE

P.O. BOX 51453, LIMBE, MALAWI

VOICE OF GOD RECORDINGS

P.O. BOX 950, JEFFERSONVILLE, INDIANA 47131 U.S.A.www.branham.org

Page 60: IYE AMENE A M Idownload.branham.org/pdf/CHA/CHA63-1110E He That Is In... · 2019-11-11 · IYEAMENEALI MWA INU Zikomoinu,M’baleNeville.Ambuyeakudalitseniinu. Tiyenitingokhalabechiimirekwamphindichabepamene

Chidziwitso kwa ofuna kusindikiza

Maufulu onse ndi osungidwa. Bukhu ili mukhoza ku printa kunyumba kwanu ngati mutafuna kuti mugwiritse ntchito inuyo kapena kuti mukawapatse ena, ulere, ngati chida chofalitsira Uthenga wa Yesu Khristu. Bukhu ili simungathe kuligulitsa, kulichulukitsa kuti akhalepo ambiri, kuikidwa pa intaneti, kukaliika pakuti ena azitengapo, kumasuliridwa mu zinenero zina, kapena kugwiritsidwa ntchito ngati njira yopezera ndalama popanda chilolezo chochita kulembedwa ndi a Voice Of God Recordings®.

Ngati mukufuna kuti mumve zambiri kapena ngati mukufuna zipangizo zina zimene tiri nazo, chonde mulembere ku:

Voice of God RecoRdinGsP.o. Box 950, JeffeRsonVille, indiana 47131 U.s.a.

www.branham.org